Pitani ku nkhani yake

Anthu Okwatirana Komanso Mabanja

Baibulo lomwe ndi buku la anthu onse limapereka malangizo omwe angathandize kuti banja lanu likhale losangalala komanso kuti mulere bwino ana anu. a

a Mu chigawo chino, tasintha maina a anthu ena omwe tawagwira mawu.

ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA

Mungatani Kuti Mupewe Kuthetsa Banja Pambuyo Pokhala Limodzi kwa Zaka Zambiri?

N’chiyani chikuchititsa kuti anthu azithetsa banja pambuyo pokhala limodzi kwa zaka zambiri? Kodi mungatani kuti zimenezi zisakuchitikireni?

ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA

Mungatani Kuti Mupewe Kuthetsa Banja Pambuyo Pokhala Limodzi kwa Zaka Zambiri?

N’chiyani chikuchititsa kuti anthu azithetsa banja pambuyo pokhala limodzi kwa zaka zambiri? Kodi mungatani kuti zimenezi zisakuchitikireni?

Kulera Ana

Laibulale

Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala

Mukhoza kukhala ndi banja losangalala mukamatsatira mfundo za m’Baibulo.