NSANJA YA MLONDA September 2015 | Mmene mungalimbanilane ndi nkhawa
Anthu mamiliyoni ambili amakumana ndi ngozi zacilengedwe, koma ena amalimbana ndi mavuto amenewa ali ndi nkhawa zocepa pamene ena amakhala ndi nkhawa zambili. Amacita bwanji zimenezo?
NKHANI YA PACIKUTO
Anthu Kulikonse Ali Ndi Nkhawa
Kafukufuku akuonetsa kuti ngakhale nkhawa yaing’ono ingacititse munthu kufa msanga. Kodi mungalimbane bwanji ndi nkhawa?
NKHANI YA PACIKUTO
Nkhawa Zokhudza Ndalama
Mwamuna wina anakwanitsa kusamalila banja lake ngakhale pamene zinthu zofunika paumoyo zinakwela mtengo kufika ku mabiliyoni.
NKHANI YA PACIKUTO
Nkhawa Zokhudza Banja
Nkhani ya mkazi wosiidwa ndi mwamuna wake, kutha kwa banja, ndi kupilila mavuto, ionetsa ubwino wokhala ndi cikhulupililo.
NKHANI YA PACIKUTO
Nkhawa Zokhudza Ngozi
Kodi mungalimbane bwanji ndi nkhondo, ciwawa, kuonongeka kwa cilengedwe, kusintha kwa nyengo, ndi milili?
BAIBO IMASINTHA ANTHU
Umoyo Wanga Unali Kuipilaipilabe
Stephen McDowell anali mnyamata waciwawa, koma kumangidwa kwa anzake amene anapha munthu, kunamucitsa kuyamba kuphunzila Baibulo.
TENGELANI CIKHULUPILILO CAWO
“Ine Ndinauka Monga Mai mu Isiraeli”
Kodi nkhani ya m’Baibulo ya Debora itiphunzitsa ciani za cikhulupililo ndi kulimba mtima?
Kuyankha Mafunso a m’Baibulo
Kodi colinga ca moyo n’ciani? N’cifukwa ciani Mulungu anapanga anthu?
Madanga Ena Opezeka pa Intaneti
Kodi Nkhondo ya Aramagedo N’ciyani?
Mawu akuti Aramagedo amapezeka kamodzi kokha m’Baibo. Koma nkhondo imene mawuwa amatanthauza imachulidwa m’Baibo lonse.