Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Nehemiya

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Nehemiya

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe mfundo zina zokhudza buku la Nehemiya. Bukuli limafotokoza za kumanganso Yerusalemu Ayuda atachoka ku ukapolo wa ku Babulo.