Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Masalimo

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Masalimo

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene zili m’buku la Masalimo. Bukuli lili ndi uthenga umene ungakulimbikitseni panopa komanso kukuthandizani kudziwa zinthu zabwino zimene Mulungu achite m’tsogolo muno.