Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Malaki

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Malaki

Onerani vidiyoyi yomwe ikufotokoza mwachidule mfundo za m’buku lomaliza m’Malemba Achiheberi. M’bukuli muli ulosi womwe umasonyeza kuti Yehova sasintha mfundo zimene amayendera, ndi wachifundo komanso wachikondi.