Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Kukwaniritsa Zolinga Zauzimu

A Mboni za Yehova aona kuti Baibulo limawathandiza kupitiriza kukhala olimba m’chikhulupiriro ndiponso kukwaniritsa zolinga zawo.

Cameron Anapeza Moyo Wabwino Kwambiri

Kodi mukufuna kukhala munthu wosangalala? Mvetserani pamene Cameron akufotokoza zimene zinamuthandiza kuti akhale wosangalala atapita kumalo amene samaganizira kuti angafikeko.

Anadzipereka ndi Mtima Wonse

Alongo ambiri amene anasamukira kumayiko ena poyamba ankadzikayikira. Kodi anatani kuti alimbe mtima? Kodi aphunzirapo chiyani atatumikira kudziko lina?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Albania ndi ku Kosovo

Kodi anapeza madalitso otani omwe awathandiza kupirira ngakhale kuti akhala akukumana ndi mavuto?

Anadzipereka Ndi Mtima Wonse ku Bulgaria

Kodi ndi mavuto otani amene anthu amakumana nawo akasamukira kudziko lina kuti akalalikire?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse—Ku Ghana

Anthu amene anasamukira m’mayiko ena amakumana ndi mavuto ambiri koma amadalitsidwanso kwabasi.

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Guyana

Kodi tingaphunzire zotani kwa anthu amene anatumikirapo kumene kukufunika olalikira ambiri? Kodi zimene iwo ananena zingakuthandizeni bwanji kukonzekera kukatumikira kudziko lina ngati mukufuna kutero?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Madagascar

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe za anthu amene adzipereka kuti akathandize kufalitsa uthenga wa Ufumu kumadera osiyanasiyana a m’dziko lalikulu la Madagascar.

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Micronesia

Anthu ochokera kumayiko ena amene akutumikira kuzilumba za m’nyanja ya Pacific zimenezi nthawi zambiri amakumana ndi mavuto atatu. Kodi amathana nawo bwanji?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Myanmar

Kodi n’chifukwa chiyani a Mboni za Yehova ambiri achoka kwawo kuti akathandize pa ntchito yolalikira ku Myanmar?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku New York

N’chiyani chinachititsa anthu okhala m’nyumba yabwino kwambiri kuti alolere kusamukira m’kanyumba kakang’ono kwambiri

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Norway

Kodi funso limene anafunsidwa mosayembekezereka linathandiza bwanji banja lina kuti lisamukire kudera limene kukufunika anthu ambiri ogwira ntchito yolalikira?

Anadzipereka Ndi Mtima Wonse ku Oceania

Kodi a Mboni za Yehova amene anasamukira komwe kulibe ofalitsa ambiri ku Oceania amatani akakumana mavuto?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Philippines

Onani zimene zinalimbikitsa anthu ena kuti asiye ntchito yawo komanso kugulitsa katundu wawo n’kukakhala kumadera akumidzi ku Philippines.

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Russia

Werengani kuti mumve za abale ndi alongo amene anasamukira ku Russia kuti akathandize. Ena ndi apabanja ena ayi ndipo onse aphunzira kudalira kwambiri Yehova.

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Taiwan

A Mboni za Yehova oposa 100 apita kukatumikira ku Taiwan. Onani mmene zinthu zikuyendera pa moyo wawo komanso zimene zikuwathandiza kutumikira bwino.

Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Turkey

Mu 2014, kunali ntchito yapadera yolalikira ku Turkey. N’chifukwa chiyani ntchito yapaderayi inachitika? Kodi zotsatirapo zake zinali zotani?

Anadzipereka ndi Mtima Wonse Kumadzulo kwa Africa

Kodi n’chiyani chinalimbikitsa Akhristu ena ku Ulaya kuti asamukire kumadzulo kwa Africa, nanga zinthu zikuwayendera bwanji kumeneko?

Tinasankha Kukhala Moyo Wosalira Zambiri

Nkhani imene inakambidwa kumsonkhano wina inathandiza banja lina la ku Colombia kuti lionenso zinthu zimene linkaika patsogolo.

Zimene Ndinasankha Ndili Mwana

Mnyamata wina wa ku Columbus, Ohio, U.S.A. anaganiza zophunzira Chikambodiya. N’chifukwa chiyani anachita zimenezi? Kodi zimenezi zinakhudza bwanji zimene anadzachita m’tsogolo?