Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Sukulu

Mukamapita kusukulu, mumayesedwa pa zinthu monga kukhala oganiza, odekha kapenanso osangalala ndiponso pa nkhani yokhala okhulupirika kwa Mulungu. Mungatani kuti mukwanitse kuphunzira bwinobwino popanda kuvutika ndi nkhawa?

Ndingatani Ngati Anzanga Amandivutitsa?

Simungathe kuchititsa kuti anthu asamakuvutitseni, koma mungathe kusintha mmene mumawayankhira.

Kodi Mungatani Kuti Anzanu Asiye Kukuvutitsani?

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe chifukwa chake anthu amavutitsa anzawo komanso zimene mungachite kuti asiye kukuvutitsani.