12
Kachisi Womangidwa ndi Solomo
-
Mbali za Kachisi
-
1 Malo Oyera Koposa (1 Maf. 6:16, 20)
-
2 Malo Oyera (2 Mbiri 5:9)
-
3 Zipinda Zakudenga (1 Mbiri 28:11)
-
4 Zipinda Zam’mbali (1 Maf. 6:5, 6, 10)
-
5 Yakini (1 Maf. 7:21; 2 Mbiri 3:17)
-
6 Boazi (1 Maf. 7:21; 2 Mbiri 3:17)
-
7 Khonde (1 Maf. 6:3; 2 Mbiri 3:4) (Kutalika kwake sikukudziwika bwinobwino)
-
8 Guwa Lansembe Lamkuwa (2 Mbiri 4:1)
-
9 Nsanja Yamkuwa (2 Mbiri 6:13)
-
10 Bwalo la Mkati (1 Maf. 6:36)
-
11 Thanki Yamkuwa (1 Maf. 7:23)
-
12 Zotengera Zamawilo (1 Maf. 7:27)
-
13 Khomo la M’mbali (1 Maf. 6:8)
-
14 Zipinda Zodyeramo (1 Mbiri 28:12)