Mwana Wamkazi Wokondedwa
Daunilodi:
1.Iwo anaona
Ali mwana.
Inde ni zambili
Adzapitamo.
Koma iye anaŵakondweletsa
Popilila ziyeso.
(KOLASI)
Iwe mwana, akunyadila.
Nthawi zonse akukonda.
2.Niwodzipeleka
Nthawi zonse.
Zonse amuuza
Amatsatila.
Ndipo amakondwela
Akamvela
Atate wake akuti;
(KOLASI)
“Mwana wanga wamkazi iwe,
Nthawi zonse n’dzakukonda.”
(BILIJI)
Yehova M’lungu adziŵa zonse,
Ndiponso khama unaonetsa.
Sadzaiŵala cikondi cako
Pom’tamanda.
(KOLASI)
Iwe mwana akunyadila.
Nthawi zonse sadzakusiya.
M’lungu adzakusamalila.
Iye amakukonda.