Kukonda Abale YAMBANI Kukonda Abale Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Pangani Dawunilodi: Manotsi 1. Kulikonse komwetu tingapite, Kuli anthu a Yehova, abale athu. Tingamvedi Kutitu Amatikonda. Chikondidi. 2. Abale akugwirizanadi Ndi Yehova komanso mwana wake Polimbitsa Ubale wa Padziko lonse. Chikondidi. (KOLASI) Atate atisamala Sangatisiye. 3. Okhala m’nkhalango ndi m’mapiri, M’matawuni ngakhale m’zilumba zonse, Nonsenu. Ndinudi anthu a Yehova. Okondedwa. (KOLASI) Atate atisamala— Sangatiiwale. (VESI LOKOMETSERA) Ngakhale dziko n’loopsa— Ndilochititsa manthadi. N’zosangalatsadi kudziwa Yehova ndi anthu ake! 4. Yesu anati tizikondana. Abale onsetu akuyesetsadi Kukondana— Inunso mukuyesetsadi. Kukondana. Kukondana. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Kukonda Abale NYIMBO ZATHU Kukonda Abale Chinenero Chamanja cha ku Malawi Kukonda Abale https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1014254/univ/art/1014254_univ_sqr_xl.jpg