Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Kufuna-funa

Kufuna-funa

Daunilodi

  1. 1. Tinayesa kusakila

    Tinacipezadi Cuma

    Tinali na mafunso pali M’lungu

    Koma tinafufuza.

    (MWANA WA KOLASI)

    Sitinaleke kufuna-funa.

    Tinadziŵa kuti tidzapeza co’nadi.

    (KOLASI)

    Ise tinasakila

    mayankho oona

    A mafunso tinafunsa.

    Kulengedwa kwathu nakufunika

    Kwa Ufumu wa M’lungu (Kufuna-funa)

  2. 2. Sitinali kudziŵa dzina ya M’lungu

    Woona Yehova

    Pamene tinaphunzila

    Tinasangalaladi

    (MWANA WA KOLASI)

    Sitinaleke kufunafuna Co’nadi

    Caciyambi na tsogolo la anthu.

    (KOLASI)

    Ise tinasakila

    Mayankho oona

    A mafunso tinafunsa.

    Kulengedwa kwathu nakufunika

    Kwa Ufumu wa M’lungu (Kufuna-funa)

    (BILIJI)

    Timathandiza ena

    Kuti acipeze co’nadi tinapeza

    Kusakila mayankho oona

    timaŵathandizila

    Kuti apeze co’nadi

    (KOLASI)

    Nawo anasakila

    mayankho oona

    A mafunso anafunsa.

    Kulengedwa kwathu, moyo wosatha

    Mu ufumu wa M’lungu (Kufuna-funa)