Nilimbitseni Mtima
(2 Mafumu 6:16)
Daunilodi:
1. Navutika mtima—
Nasoŵa cocita.
Olo zinthu zinivute;
Mumanithandiza.
Moyo ungavute,
Koma nimadziŵa:
Ndimwe wokhulupilika;
Mudzaniteteza.
(KOLASI)
Yehova, nithandizeni
Kuti niziona.
Tilidi ambili kuposa
Olimbana nafe.
Conde, n’thandizeni;
Kuti nipilile.
Nilimbitseni mtima,
Simungalephele.
2. Ndine cabe munthu.
Nimacita mantha.
Ndimwe pothaŵila panga;
Simumalephela.
Munipatse mphamvu,
Kuti nisayope.
Ine nidzapililabe—
Kufikila imfa.
(KOLASI)
Yehova, nithandizeni
Kuti niziona.
Tilidi ambili kuposa
Olimbana nafe.
Conde, n’thandizeni;
Kuti nipilile.
Nilimbitseni mtima,
Simungalephele.
(KOLASI)
Yehova, nithandizeni
Kuti niziona.
Tilidi ambili kuposa
Olimbana nafe.
Conde, n’thandizeni;
Kuti nipilile.
Nilimbitseni mtima,
Simungalephele.
Nilimbitseni mtima,
Simungalephele.