Tsiku Lililonse Lili N’zodetsa Nkhawa Zake YAMBANI Tsiku Lililonse Lili N’zodetsa Nkhawa Zake Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Pangani Dawunilodi: Manotsi 1.Za dziko latsopano ndikudziwa ndithu, Ndikukhulupiriradi mavuto adzatha. Koma pena ndi zovuta, Kuona malonjezowo, Ndi chikondi cha Mulungu ndikakhala m’mavuto. Koma Yehova ’lipo. (KOLASI) Ndimapemphera kwa M’lungu. Ndikakhalatu ndi nkhawa, N’dalire mphamvu zake. Yehovatu ali nane. Wandipatsa mawuwa. Ndi anzanga abwino. Tsiku lililonse lili n’zake. Ndiye ndisadzitopetse, Ndisaganizire zamawa. Zamawa n’zina Ndisade nkhawa. 2. Mvera malangizo anga, Ndimakukonda. Ganizira zabwino, Osati mavutowa. Zomwe M’lungu wachita. Anaperekatu Yesu. Um’khulupirire ndithu. Watipatsatu zambiri. Ndiye usaope. (KOLASI) Tim’pemphe Yehova. Tikakhalatu ndi nkhawa, Timudalire ndithu. Yehovatu ali nafe. Watipatsa mawuwa Ndi anzathu abwino. Tsiku lililonse lili n’zake Ndiye tisadzitopetse. Tisaganizire zamawa; Zamawa n’zina; Tisade nkhawa. (KOLASI) Tim’pemphe Yehova. Tikakhalatu ndi nkhawa, Timudalire ndithu. Yehova ali nafe. Watipatsa mawuwa Ndi anzathu abwino. Tsiku lililonse lili n’zake. Ndiye usadzitopetse; Usaganizire zamawa. Zamawa n’zina Usade nkhawa— Tisade nkhawa. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Tsiku Lililonse Lili N’zodetsa Nkhawa Zake NYIMBO ZATHU Tsiku Lililonse Lili N’zodetsa Nkhawa Zake Chinenero Chamanja cha ku Malawi Tsiku Lililonse Lili N’zodetsa Nkhawa Zake https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1014309/univ/art/1014309_univ_sqr_xl.jpg