Dziko Latsopano Lomwe Likubwera YAMBANI Dziko Latsopano Lomwe Likubwera Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi Pangani Dawunilodi: Manotsi 1. M’maganizo taonani izi: Mukuona zinthu zochititsa chidwi Ana ‘kusewera M’dziko lomwe nkhawa zonse zatha. Anthu onse okhulupirika Akusamalira bwino dzikoli. Kulitu chitetezo— Ndi mtendere mpaka kalekale. N’zosangalatsa, Yesu akulamulira M’dziko latsopano. (KOLASI) Chiyembekezo chathu Chili ngati nangula wathu, Chimawala ngatitu dzuwa Ngatitu tilidi M’dziko latsopano. 2. Taganizirani malo ake Mapiri, mitsinje, malo okongola. Uku ndiye kwanu. Mukutuluka m’nyumba mwanu, Pali wina wom’dziwa Wofunika kum’kumbatira Tikusangalala— Padutsa zaka osamuona Imfa yagonja N’chikondi chake M’dziko latsopano. (KOLASI) Chiyembekezo chathu Chili ngati nangula wathu, Chimawala ngatitu dzuwa Ngatitu tilidi M’dziko latsopano. (VESI LOKOMETSERA) Mawu onse wanena Adzakwaniritsidwa ndithu. N’chifuniro cha Yehova Watipatsa zonse tinkafuna. (KOLASI) Chiyembekezo chathu Chili ngati nangula wathu, Chimawala ngatitu dzuwa Ngatitu tilidi M’dziko latsopano, M’dziko latsopano, M’dziko latsopano, M’dziko latsopano. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Dziko Latsopano Lomwe Likubwera NYIMBO ZATHU Dziko Latsopano Lomwe Likubwera Chinenero Chamanja cha ku Malawi Dziko Latsopano Lomwe Likubwera https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1014323/univ/art/1014323_univ_sqr_xl.jpg