Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Tsimikizani

Tsimikizani

Pangani Dawunilodi:

  1. 1. Mumapemphera.

    M’malalikira.

    Mwakhulupirika muzonse.

    Mayesero anu ndi ambiridi,

    Koma Yehova akuona.

    (KUKONZEKERA KOLASI)

    Mukamaweruzidwa kumakhoti,

    Simuli nokha.

    Ndinutu zitsanzo zabwino,

    N’zolimbikitsa.

    (KOLASI)

    ‘Ndatsimikiza

    Imfa, moyo, maboma satilekanitsa ndi M’lungu.’

    ‘Ndatsimikiza

    Zam’tsogolo, kaya mphamvu, sizitilekanitsa.’

    Tsimikizani

    Kukondabe M’lungu.

  2. 2. Mwachita bwino.

    Simunagonje.

    M’madalira M’lungu

    Nthawi zonse.

    Adani ayesa kutiletsatu,

    Dziwani tili mbali yanu.

    (KUKONZEKERA KOLASI)

    Mukamaweruzidwa kumakhoti,

    Simuli nokha.

    Ndinutu zitsanzo zabwino,

    N’zolimbikitsa.

    (KOLASI)

    ‘Ndatsimikiza

    Imfa, moyo, maboma satilekanitsa ndi M’lungu.’

    ‘Ndatsimikiza

    Zam’tsogolo, kaya mphamvu, sizitilekanitsa.’

    Tsimikizani

    Kukondabe M’lungu.

    Mudziwetu.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Tikhoza kuzunzidwa pomvera Mulungu—

    Pokonda M’lungu.

    ‘Komabetu mukugonjetsa zinthu zonsezi’—

    Simunagonje.

    (KOLASI)

    ‘Ndatsimikiza

    Imfa, moyo, maboma satilekanitsa ndi M’lungu.’

    ‘Ndatsimikiza

    Zam’tsogolo, kaya mphamvu, sizitilekanitsa.’

    ‘Ndatsimikiza

    Imfa, moyo, maboma satilekanitsa ndi M’lungu.’

    ‘Ndatsimikiza

    Zam’tsogolo, kaya mphamvu, sizitilekanitsa.’

    Tsimikizani

    Kukondabe M’lungu.