Cimwemwe Cathu Camuyaya
(Salimo 16:11)
Daunilodi:
1. Kumwamba kuli nyenyezi ndipo ziwala.
Munakongoletsa usana na usiku.
Manja anu anapanga zinthu zonse,
Mukondwela mukaziona.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga waufumu,
Zimatikondweletsa.
Cikondi canu cosatha,
Ndiye cuma camuyaya
Ndimwe cimwemwe cathu.
Inde, ca muyaya.
2. Yehova tili na zonse zosangalatsa.
Zonse tiona na maso, zikhudza mtima.
Mwatipatsa umuyaya,
Mumitima yathu na cimwemwe cosatha.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga waufumu,
Zimatikondweletsa.
Cikondi canu cosatha,
Ndiye cuma camuyaya
Ndimwe cimwemwe cathu.
Inde, ca muyaya.
(BILIJI)
Munapeleka Yesu
Kuti atifele
Sitikanapeza cimwemwe
Popanda nsembe yake.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga waufumu,
Zimatikondweletsa.
Cikondi canu cosatha
Ndiye cuma camuyaya.
Ndimwe cimwemwe cathu
Inde, ca muyaya.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga waufumu,
Zimatikondweletsa
Cikondi canu cosatha
Ndiye cuma camuyaya
Ndimwe cimwemwe cathu
Inde, ca muyaya.
(Onaninso Sal. 37:4; 1 Akor. 15:28.)