Kudzakhala Mtendere (Nyimbo ya Msonkhano ya 2022)
Pangani Dawunilodi:
1. Pomwe dziko likusowa mtendere
Ife tili ndi mtendere.
Sitida nkhawa
Chifukwa Yehova
Adzathetsatu mavuto.
(KOLASI)
Padziko lapansi
Padzakhalatu
Mtendere wosatha.
Mavuto akatha,
Tidzapumula.
Konse kudzakhala
Mtendere.
2. Tikalowa m’dziko
Latsopano
Moyo udzasangalatsa.
Mtendere womwe
Tikulakalaka
Yehova adzatipatsa.
(KOLASI)
Padziko lapansi
Padzakhalatu
Mtendere wosatha.
Mavuto akatha,
Tidzapumula.
Konse kudzakhala
Mtendere.
(KOLASI)
Padziko lapansi
Padzakhalatu
Mtendere wosatha.
Mavuto akatha,
Tidzapumula.
Tidzasangalala!
(KOLASI)
Padziko lapansi
Padzakhalatu
Mtendere wosatha.
Mavuto akatha,
Tidzapumula.
Konse kudzakhala
Mtendere,
Mtendere!