Moyo Wosatha
Pangani Dawunilodi:
1. M’dzikoli ndi zovuta
Kuti usiyanitse
Zabwinotu ndi zoipa.
(KUKONZEKERA KOLASI)
Komatu Yehova akuti: ‘Pewa nzeru za dziko’.
Upeza moyo wosathadi.
(KOLASI)
Pirira, pemphera.
Yehova ali nawe, sulitu wekha.
Ndiye limbabe.
Mavuto angakule, akuthandiza.
Ganiza za moyo, moyo wosatha.
2. Dzikoli likufuna
Ukhale wodziwika
Kwa anthu, utchuketu.
(KUKONZEKELA KOLASI)
Koma ndi zachabechabe, ndi kuthamangitsa mphepo.
Ndiye ganiza za mtsogolo.
(KOLASI)
Pirira, pemphera.
Yehova ali nawe, sulitu wekha.
Ndiye limbabe.
Mavuto angakule akuthandiza.
Ganiza za moyo, moyo wosatha
(KOLASI)
Pirira, pemphera.
Yehova ali nawe, sulitu wekha.
Ndiye limbabe.
Mavuto angakule, akuthandiza.
Ganiza za moyo, moyo wosatha.