Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Tisafooke

Tisafooke

Pangani Dawunilodi:

  1. 1. Nthawi yafupika

    Dziko liwonongedwa.

    Koma anthu adziwa bwanji?

    Tiwalalikire.

  2. 2. Tisakhale chete.

    Tisamachite mantha.

    Tidaliretu M’lungu wathu

    Azitithandiza.

    (KOLASI)

    Ngati moto woyaka

    Tizilalikira.

    Inde! Tisafo’ke.

    Tisamanyalanyaze

    Tidziwitse onse.

    Inde! Tisafo’ke.

    Tisafo’ke.

  3. 3. Tizichita khama.

    Nthawiyi yafupika.

    Tiliyeretse dzina lake.

    Tidzasangalala.

    (KOLASI)

    Ngati moto woyaka

    Tizilalikira.

    Inde! Tisafo’ke.

    Tisamanyalanyaze

    Tidziwitse onse.

    Inde! Tisafo’ke.

    Tisafo’ke.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Moto uziyakatu mumtima mwathu.

    Tsiku la Yehova likubwera

    Posachedwa.

    (KOLASI)

    Ngati moto woyaka

    Tizilalikira.

    Inde! Tisafo’ke.

    Tisamanyalanyaze

    Tidziwitse onse.

    Inde! Tisafo’ke.

    Tisafo’ke.

    Tisafo’ke.

    Tisafo’ke.