Tisafooke
Pangani Dawunilodi:
1. Nthawi yafupika
Dziko liwonongedwa.
Koma anthu adziwa bwanji?
Tiwalalikire.
2. Tisakhale chete.
Tisamachite mantha.
Tidaliretu M’lungu wathu
Azitithandiza.
(KOLASI)
Ngati moto woyaka
Tizilalikira.
Inde! Tisafo’ke.
Tisamanyalanyaze
Tidziwitse onse.
Inde! Tisafo’ke.
Tisafo’ke.
3. Tizichita khama.
Nthawiyi yafupika.
Tiliyeretse dzina lake.
Tidzasangalala.
(KOLASI)
Ngati moto woyaka
Tizilalikira.
Inde! Tisafo’ke.
Tisamanyalanyaze
Tidziwitse onse.
Inde! Tisafo’ke.
Tisafo’ke.
(VESI LOKOMETSERA)
Moto uziyakatu mumtima mwathu.
Tsiku la Yehova likubwera
Posachedwa.
(KOLASI)
Ngati moto woyaka
Tizilalikira.
Inde! Tisafo’ke.
Tisamanyalanyaze
Tidziwitse onse.
Inde! Tisafo’ke.
Tisafo’ke.
Tisafo’ke.
Tisafo’ke.