Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zisonyezero za Voliyumu 81 ya Galamukani!

Zisonyezero za Voliyumu 81 ya Galamukani!

Zisonyezero za Voliyumu 81 ya Galamukani!

ACHINYAMATA AKUFUNSA

Angathaŵedi Ana Awo, 6/8, 12/8

Kodi Ndikhale ndi Khadi la Ngongole? 1/8

Kodi Ndisamukire Kudziko lina? 7/8

Kubereka Ana, 5/8

Kuboola Thupi, 4/8

Kuvutika Maganizo, 11/8

Kuvutitsidwa ndi Amuna Kapena Akazi, 9/8

N’chifukwa Chiyani Bwenzi Langa Linandikhumudwitsa? 3/8

N’chifukwa Chiyani Ndili Wochepa Thupi? 10/8

CHIPEMBEDZO

‘Iwo Anali Osangalatsa,’ 1/8

Kukhulupirira Mizimu—N’kothandiza Kapena N’kovulaza? 8/8

Pali zinthu zambiri zimene maso paokha sangaone, 9/8

CHUMA NDI NTCHITO

Kodi “Ntchito Yokhazikika” Idamka Kuti? 10/8

LINGALIRO LA BAIBULO

Chikhulupiriro Choona N’chiyani? 3/8

Kodi Kulambira Yesu N’koyenera? 4/8

Kodi Mulungu Amasandulika? 6/

Kodi Sayansi Ingabweretse Moyo Wosatha? 12/8

Kudzikongoletsa, 8/8

Kunama—Kodi Nthaŵi Zina N’kolungama? 2/8

Kusinkhasinkha Kumene Kumapindulitsa, 9/8

“Maseŵera Angozi,” 10/8

Njira Yogonjetsera Kutaya Mtima, 5/8

Nyenyezi Zolosera, 11/8

MAUNANSI A ANTHU

Kodi Chisoni Chiyenera Kusonyezedwa? 8/8

Mabanja Opanda Bambo, 2/8

Mmene Banja Lathu Linagwirizanirananso, 6/8

Mwetulirani—N’zothandiza kwa Inu! 7/8

Kuona Miyambo Yotchuka M’njira Yoyenera, 1/8

MAYIKO NDI ANTHU

AIDS mu Afirika, 5/8

Amayi Odwala AIDS Akusowa Pogwira, 1/8

Chivomezi! (Taiwan), 9/8

Thandizo kwa Ozunzidwa [Denmark], 1/8

MBONI ZA YEHOVA

Anawapulumutsa Lokumbakumba (Benin), 11/8

Anthu a ku Russia Akuyamikira Ufulu wa Kulambira, 3/8

Chikhulupiriro Cholimba M’kati mwa Mavuto (P. Esch), 4/8

Kuthandiza Achinyamata Kusiya Kupulupudza (France), 9/8

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Chimene Ndimaikirapo Mtima Kwambiri Ndicho Kukhalabe Wokhulupirika (A. Davidjuk), 10/8

Khama Langa Lofuna Kusankha Zinthu Mwanzeru (G. Sisson), 9/8

Kukhalabe Okhulupirika mu Ulamuliro Wankhanza (M. Dasevich), 10/8

Kuthana ndi Ziyeso Mwamphamvu ya Mulungu (S. Kozhemba), 12/8

Kuyesedwa kwa Chikhulupiriro ku Poland (J. Ferenc), 11/8

Loida Ayamba Kulankhula, 5/8

Ngakhale Ndili Wolumala Ndine Wosangala (K. Morozov), 12/8

SAYANSI

Kupanga Mapu Osonyeza Miyamba, 2/8

Thambo Lathu—Kodi Linangokhalako Mwamwayi? 10/8

Zimene Diso Palokha Silingaone, 9/8

UMOYO NDI MANKHWALA

AIDS mu Afirika, 5/8

Amayi Odwala AIDS Akusowa Pogwira, 1/8

Anamwino, 11/8

Chithandizo ndi Opaleshoni Zopanda Magazi, 1/8

Kodi Ndizimwa Asipilini Tsiku N’tsiku? 7/8

N’kusiyiranji Kusuta, 4/8

Kuthana ndi Matenda a Kachiwalo Kotchedwa Prostate, 12/8

Matenda Aakulu, 6/8

Mliri wa Matenda a Makoswe, 2/8

Mukadwala Chifukwa cha Mankhwala, 8/8

Njira Zochiritsira, 11/8

“Ufa!” (nkhani ya magazi), 5/8

ZINYAMA NDI ZOMERA

Kamzimbi (Mbalame), 2/8

Kodi Mbalame Ingam’phunzitsenji Mkaidi? 5/8

Mtundu Wodabwitsa wa Mbalame, 8/8

Nyamalikiti, 10/8

Nzimbe, 8/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE

Anthu Ovutika ndi Nkhondo Asintha, 2/8

Kodi kuona zithunzi zamaliseche pa intaneti kuli n’zoopsa zanji? Kodi zimenezi n’kuzipeŵa motani? 6/8

Kodi Makhalidwe ndi Otani Lerolino? 4/8

Kodi Moyo Ukutsikiratsikira Mtengo? 7/8

Kudzipha—Mliri Wobisika, 3/8

Kufuna Kuchotsa Boma la Vatican M’bungwe la UN, 11/8

Kusiyana Pakati pa Olemera ndi Osauka Kukukula, 2/8

Mabanja Opanda Bambo, 2/8

Mabomba Okwirira Pansi, 5/8

Malonda a Kuba Anthu, 1/8

Mavuto a Ana, 12/8

Nkhani Zokopa Zingaphetse Anthu, 7/8

Ukapolo Wamakono, 3/8

Zolinga za Olimpiki Zakanika? 9/8

ZOSIYANASIYANA

El Niño? 4/8

Kumeta Moyeretsa, 2/8

Nkhani za pa TV, 5/8

Zoopsa za Kukwera Matola, 7/8