Mtendere Komanso Moyo Wosangalala
Baibulo lathandiza anthu ambirimbiri kupirira mavuto, kuchepetsako nkhawa komanso kuthana ndi mavuto ena ndipo lawathandizanso kuona kuti moyo uli ndi cholinga.
Zina Zimene Zilipo
Onerani Baibulo pa Intaneti
Onani zimene zili mu Baibulo la Dziko Latsopano lomwe ndi lolondola komanso losavuta kuwerenga.
Onerani Baibulo pa Intaneti
Onani zimene zili mu Baibulo la Dziko Latsopano lomwe ndi lolondola komanso losavuta kuwerenga.
Sankhani Nkhani Imene Yakusangalatsani
Yambani kuphunzira Baibulo
Phunzirani Baibulo kwaulere, mochita kukambirana ndi mphunzitsi wanu.
Pemphani Kuti Tidzakuyendereni
Mutha kukhala ndi mwayi wokambirana nkhani inayake ya m’Baibulo kapena kudziwa zambiri zokhudza Mboni za Yehova.
Fikani Pamsonkhano
Dziwani zambiri zokhudza misonkhano yathu. Pezani malo apafupi amene kumachitikira misonkhano yathu.
Mavidiyo
Kodi Mulungu Amavomereza Zipembedzo Zonse?
Anthu amaganiza kuti palibe vuto ngati munthu atalowa m’chipembedzo chilichonse.