Chikuto Chakumbuyo
Chikuto Chakumbuyo
Zigawo za bukuli zili ndi mitu iyi
KUKHALA NDI MAKOLO KOMANSO ACHIBALE
KUGONANA, MAKHALIDWE NDIPONSO CHIKONDI
MAKHALIDWE AMENE ANGAWONONGE MOYO WANU
ZIMENE MUMACHITA PA NTHAWI YOPUMA
MAWU AKUMAPETO OPITA KWA MAKOLO
Malangizo othandiza achinyamata. Kodi n’chiyani chingakuthandizeni kuti mukhale ndi makhalidwe abwino omwe angadzakuthandizeni mukadzakula? Buku Loyamba la Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, lingakuthandizeni. Malangizo amene ali m’bukuli ndi ogwirizana ndi mfundo za m’Baibulo. Mawu a Mulungu athandiza anthu mamiliyoni ambiri kulimbana ndi mavuto pa moyo wawo. Werengani bukuli kuti muone mmene lingakuthandizireni.
“Kuganiza bwino kudzakuyang’anira, ndipo kuzindikira kudzakuteteza.”—Miyambo 2:11.