Pitani ku nkhani yake

Phunziro 1: Muzimvera Makolo Anu

Phunziro 1: Muzimvera Makolo Anu

N’chifukwa chiyani tiyenera kumvera makolo athu? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene zinathandiza Kalebe kuti aone chifukwa chake tiyenera kumvera makolo.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.