Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Muzipemphera Nthawi Iliyonse: Nyimbo ndi Mawu Ake

Muzipemphera Nthawi Iliyonse: Nyimbo ndi Mawu Ake

Pangani dawunilodi tsamba la nyimboli, ndipo muimbe limodzi ndi Sofiya. Mudziwanso nthawi komanso malo amene mungapemphere.

 

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Muzipemphera Nthawi Iliyonse

Vidiyoyi ndi yoti mukhoza kuipanga dawunilodi ndipo imaphunzitsa ana nthawi komanso malo amene angapemphere kwa Yehova.

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.