Muzipemphera Nthawi Iliyonse: Nyimbo ndi Mawu Ake
Pangani dawunilodi tsamba la nyimboli, ndipo muimbe limodzi ndi Sofiya. Mudziwanso nthawi komanso malo amene mungapemphere.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Muzipemphera Nthawi Iliyonse
Vidiyoyi ndi yoti mukhoza kuipanga dawunilodi ndipo imaphunzitsa ana nthawi komanso malo amene angapemphere kwa Yehova.
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.