Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pangani Chikwama cha mu Utumiki

Pangani Chikwama cha mu Utumiki

Pangani dawunilodi tsambali, ndipo muonere vidiyo yakuti “Tiyeni Tikalalikire.” Kenako lumikizani tizidutswa ta chikwama cha mu utumiki tomwe tili patsambali.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Tiyeni Tikalalikire

Kodi Sofiya watenga zonse zofunika popita kolalikira? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene inunso muyenera kutenga popita kolalikira.

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Kukonzekera Kupita Kolalikira

Kodi mungasankhe zovala zimene Kalebe ndi Sofiya akufunika kuvala pokalalikira?

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.