Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Phunziro 10: Uzikhala Wokoma Mtima Ndiponso Wopatsa

Phunziro 10: Uzikhala Wokoma Mtima Ndiponso Wopatsa

Kalebe ndi Sofiya akuphunzira kufunika kogawana zinthu ndi ena. Kodi nanunso mumagawana zinthu ndi ena?

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Panga Galimoto ya Kalebe

Sindikiza, dula ndi kulumikiza galimoto ya Kalebe.

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.