Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Phunziro 13: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima

Phunziro 13: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima

Kodi munayamba mwachitapo mantha kuuza munthu zokhudza Yehova? Kodi Yehova angakuthandizeni bwanji kuti mukhale wolimba mtima?

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Posita: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima

Panga dawunilodi n’kupulinta posita ya vidiyoyi imene ingakukumbutse kuti Yehova akuthandiza kuti ukhale wolimba mtima.

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Kodi Yehova Angakuthandize Bwanji Kuti Ukhale Wolimba Mtima?

Yehova angakuthandize ngati mmene anathandizira kamtsikana ka ku Isiraeli.

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.