Phunziro 13: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima
Kodi munayamba mwachitapo mantha kuuza munthu zokhudza Yehova? Kodi Yehova angakuthandizeni bwanji kuti mukhale wolimba mtima?
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.