Kodi Zithunzizi Zikusiyana Pati?: Zochita Zokhudza Misonkhano
Pezani zinthu zomwe zikusiyana pa zithunzi ziwirizi. Kodi ndi chithunzi chiti chimene chikusonyeza khalidwe limene muyenera kusonyeza?
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Tigwire Ntchito Mogwirizana (Nyimbo Nambala 53)
Onani mmene abale athu amachitira zinthu mogwirizana pamsonkhano wa mayiko.
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.