Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Nyimbo 139

Aphunzitseni Kucilimika

Aphunzitseni Kucilimika

Daunilodi

(Mateyu 28:19, 20)

  1. Tikondwa kuphunzitsa anthu

    Okonda coonadi.

    Onani mmene akulila

    M’njila ya coonadi.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muwasamale.

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

  2. Tinali kuwapemphelela

    M’mavuto awo onse.

    Tinali kuwasamalila

    Yehova ‘wadalitsa.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muwasamale.

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

  3. Akhale odalila M’lungu,

    Na Mwana wake Yesu.

    Amvele ndipo apilile

    Tifuna apambane.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muwasamale.

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

(Onaninso Luka 6:48; Mac. 5:42; Afil. 4:1.)