Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

NYIMBO 67

“Lalikila Mau”

“Lalikila Mau”

(2 Timoteyo 4:2)

  1. 1. Mulungu watilamula

    Kuti tilalikile uthenga.

    Tilengeze kwa anthu onse,

    Adziŵe ciyembekezo cathu.

    (KOLASI)

    Lalikila,

    Kuti onse amvele!

    Lalika,

    Mapeto ayandika.

    Lalika,

    Ofatsa adzamvela.

    Lalika,

    Konse konse!

  2. 2. Anthu ena angaseke,

    Olo angafune kutitsutsa.

    Yehova adzatithandiza,

    Kuti tilalikile kwa onse.

    (KOLASI)

    Lalikila,

    Kuti onse amvele!

    Lalika,

    Mapeto ayandika.

    Lalika,

    Ofatsa adzamvela.

    Lalika,

    Konse konse!

  3. 3. Nthawi zina tidzapeza

    Ofuna kumvetsela uthenga.

    Iwo adzapulumukadi

    Tikaŵaphunzitsa coonadi.

    (KOLASI)

    Lalikila,

    Kuti onse amvele!

    Lalika,

    Mapeto ayandika.

    Lalika,

    Ofatsa adzamvela.

    Lalika,

    Konse konse!

(Onaninso Mat. 10:7; 24:14; Mac. 10:42; 1 Pet. 3:15.)