Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

NYIMBO 77

Kuwala m’Dziko la Mdima

Kuwala m’Dziko la Mdima

(2 Akorinto 4:6)

  1. 1. Kuwala kukuunika,

    m’Dziko la mdimali.

    Tiuza anthu uthenga,

    Wa ciyembekezo.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Umawala kwambili,

    m’Dziko la mdimali—

    Umapatsa anthu,

    Onse ciyembekezo—

    Mwa Mulungu.

  2. 2. Ogona agalamuke,

    Si nthawi yogona.

    Auke, tiŵalimbitse.

    Tiŵapemphelele.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu

    Umawala kwambili,

    m’Dziko la mdimali—

    Umapatsa anthu,

    Onse ciyembekezo—

    Mwa Mulungu.

(Onaninso Yoh. 3:19; 8:12; Aroma 13:11, 12; 1 Pet. 2:9.)