NYIMBO 77
Kuwala m’Dziko la Mdima
(2 Akorinto 4:6)
-
1. Kuwala kukuunika,
m’Dziko la mdimali.
Tiuza anthu uthenga,
Wa ciyembekezo.
(KOLASI)
Uthenga wa M’lungu
Umawala kwambili,
m’Dziko la mdimali—
Umapatsa anthu,
Onse ciyembekezo—
Mwa Mulungu.
-
2. Ogona agalamuke,
Si nthawi yogona.
Auke, tiŵalimbitse.
Tiŵapemphelele.
(KOLASI)
Uthenga wa M’lungu
Umawala kwambili,
m’Dziko la mdimali—
Umapatsa anthu,
Onse ciyembekezo—
Mwa Mulungu.
(Onaninso Yoh. 3:19; 8:12; Aroma 13:11, 12; 1 Pet. 2:9.)