Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

NYIMBO 119

Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba

Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba

(Aheberi 10:​38, 39)

  1. 1. Kale Mulungu ankalankhula

    Kudzera mwa aneneri.

    Pano kudzera mwa Mwana wake

    Akuti: ‘Lapanitu.’

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

  2. 2. Timamvera lamulo la Yesu

    Loti tizilalikira.

    Tilengezabe molimba mtima,

    Anthu amve uthenga.

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

  3. 3. Talimbitsa chikhulupiriro

    Sitidzabwerera m’mbuyo.

    Tikudziwa kuti M’lungu wathu

    Adzatipulumutsa.

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.