NYIMBO 138
Kukongola kwa Imvi
(Miyambo 16:31)
-
1. Pakati pathu pali
Acikulile.
Ngakhale avutike,
Iwo safo’ka.
Ena anafeledwa.
Ena adwala.
Yehova tipemphela,
Atonthozeni.
(KOLASI)
Atate Yehova,
Adalitseni.
Auzeni kuti:
“Mwagwila nchito.”
-
2. A imvi olungama
Ni okongola.
Yehova aŵakonda
Sadzaŵasiya.
Tiziŵayamikila
Pa nchito zawo.
Anadzipelekadi
Na mphamvu zonse.
(KOLASI)
Atate Yehova,
Adalitseni.
Auzeni kuti:
“Mwagwila nchito.”
(Onaninso Sal. 71:9, 18; Miy. 20:29; Mat. 25:21, 23; Luka 22:28; 1 Tim. 5:1.)