Mukamamvera Uphungu Mudzakhala Anzeru
A Byong Soo akumvetsera malangizo a m’Malemba ngakhale kuti mkulu amene akuwapatsa malangizoyo ndi wachinyamata. A Soo akumvetsera chifukwa akudziwa kuti malangizowo akuchokera kwa Yehova.
A Byong Soo akumvetsera malangizo a m’Malemba ngakhale kuti mkulu amene akuwapatsa malangizoyo ndi wachinyamata. A Soo akumvetsera chifukwa akudziwa kuti malangizowo akuchokera kwa Yehova.