Kufooka
Kodi pangakhale vuto lanji ngati atumiki a Yehova atafooka?
N’chifukwa chiyani tingakhale otsimikiza kuti Yehova adzatithandiza kulimbana ndi zinthu zofooketsa?
Sl 23:1-6; 113:6-8; Yes 40:11; 41:10, 13; 2Ak 1:3, 4
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
Mt 11:28-30—Yesu yemwe amatsatira Atate ake mosalakwitsa kanthu ndi wachifundo komanso wotsitsimula
Mt 12:15-21—Yesu anakwaniritsa ulosi wa pa Yesaya 42:1-4, pokomera mtima anthu ofooka
Malemba othandiza kulimbana ndi zinthu zomwe zingatichititse kuti tikhumudwe
Onani “Chitonthozo”
N’chifukwa chiyani tiyenera kulimbikitsa ena?
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
Nu 32:6-15—Amuna osakhulupirika 10 amene anakazonda dziko la Kanani anafooketsa Aisiraeli ndipo mtundu wonsewo unakumana ndi mavuto
2Mb 15:1-8—Uthenga wochokera kwa Yehova unathandiza Mfumu Asa kuchita zinthu molimba mtima pothana ndi khalidwe lachiwerewere