Kuwolowa Manja
Miy 11:25; Mac 20:35; 2Ak 9:11
Onaninso Miy 19:17; Mt 10:8; Lu 6:38
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
1Mb 22:6-16—Mfumu Davide anapereka mowolowa manja zinthu zothandizira kumanga kachisi ngakhale kuti sanaloledwe kumanga nawo
1Mf 17:8-16—Mkazi wamasiye wa ku Zarefati anapatsa mneneri Eliya chakudya ngakhale kuti chinali chomwecho chimene akanadya iyeyo ndi mwana wake