Ubwino
Kodi timadziwa bwanji kuti Yehova ndi wabwino?
Onaninso Yer 31:12, 13; Zek 9:16, 17
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
Eks 33:17-20; 34:5-7—Yehova anasonyeza mneneri Mose masomphenya omwe anamuthandiza kuzindikira kuti Yehova ndi wabwino, ndipo anamvanso za makhalidwe a Yehova ambiri odabwitsa
Mko 10:17, 18—Yesu ananena kuti chinthu chilichonse chabwino chimachokera kwa Yehova ndipo Iye ndi amene ali woyenera kutiuza zomwe ndi zabwino
N’chifukwa chiyani tiyenera kukhala ndi khalidwe la ubwino?