Kunama
Kodi Yehova amaona bwanji anthu omwe sasunga malonjezo awo?
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
Eks 9:27, 28, 34, 35—Farao analola kuti anthu a Mulungu apite, koma kenako anasintha maganizo ake
Eze 17:11-15, 19, 20—Yehova analanga Mfumu Zedekiya chifukwa chonyoza lumbiro lake ndiponso chifukwa chophwanya pangano lake ndi mfumu ya Babulo
Mac 5:1-10—Hananiya, ndi mkazi wake Safira, ananama kuti apereka kumpingo ndalama zonse zimene anapeza atagulitsa munda wawo
Kodi Yehova amaona bwanji anthu amiseche?
Sl 15:1-3; Miy 6:16-19; 16:28; Akl 3:9
Onaninso Miy 11:13; 1Ti 3:11
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
2Sa 16:1-4; 19:24-30—Ziba ananena zinthu zabodza zokhudza mbuye wake wokhulupirika Mefiboseti
Chv 12:9, 10—Mdyerekezi, kapena kuti Woneneza, amaneneza atumiki a Mulungu nthawi ndi nthawi