Kudzikuza
Onaninso Miy 21:24
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
2Sa 6:6, 7—Uza anachita zinthu modzikuza pogwira Likasa la Mulungu womwe sunali udindo wake; choncho Mulungu anamupha pomwepo chifukwa chochita zinthu mopanda ulemu
2Mb 26:16-21—Mfumu Uziya analangidwa chifukwa cha mtima wake wodzikuza