Kodi n’zotheka kukapeza moyo wamuyaya wacisangalalo?
Kodi mungayankhe kuti . . .
inde?
iyai?
olo kapena?
ZIMENE BAIBO IMAKAMBA
“Olungama adzalandila dziko lapansi, ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya.” —SALIMO 37:29.
UBWINO WOKHULUPILILA ZIMENEZI
Tsogolo lokondweletsa komanso la mtendele ku banja lanu na mabwenzi anu. —YEREMIYA 29:11.
Kukondwela na moyo, osati kwa kanthawi koma kwamuyaya.—SALIMO 22:26.
KODI TINGAKHULUPILILEDI ZIMENE BAIBO IMALONJEZA?
Inde! Kuti mupeze cifukwa cake, onani maumboni atatu amene ali m’kabuku kano. Mitu yake ni iyi: