Loweruka
“Tsiku ndi tsiku muzilengeza uthenga wabwino wa chipulumutso chake”—Salimo 96:2
M’mawa
8:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo
8:30 Nyimbo Na. 53 Komanso Pemphero
8:40 ‘Ndikuyenera . . . Kulengeza Uthenga Wabwino wa Ufumu’ (Luka 4:43)
8:50 VIDIYO:
Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 1
Kuwala Kwenikweni kwa Dziko—Mbali Yachiwiri (Mateyu 2:1-23; Luka 2:1-38, 41-52; Yohane 1:9)
9:25 Nyimbo Na. 69 Komanso Zilengezo
9:35 NKHANI YOSIYIRANA: Kukwaniritsidwa kwa Maulosi Onena za Mesiya
• Kunabwera Mthenga Iye Asanabwere (Malaki 3:1; 4:5; Mateyu 11:10-14)
• Anabadwa kwa Namwali (Yesaya 7:14; Mateyu 1:18, 22, 23)
• Anabadwira ku Betelehemu (Mika 5:2; Luka 2:4-7)
• Anatetezedwa Ali Mwana (Hoseya 11:1; Mateyu 2:13-15)
• Anatchedwa Mnazareti (Yesaya 11:1, 2; Mateyu 2:23)
• Anaonekera pa Nthawi Yoikidwiratu (Danieli 9:25; Luka 3:1, 2, 21, 22)
10:40 NKHANI YA UBATIZO: Pitirizani ‘Kugonjera Uthenga Wabwino’ (2 Akorinto 9:13; 1 Timoteyo 4:12-16; Aheberi 13:17)
11:10 Nyimbo Na. 24 Komanso Kupuma
Masana
12:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo
12:45 Nyimbo Na. 83
12:50 NKHANI YOSIYIRANA: Muzigwiritsa Ntchito Uthenga Wabwino Kuti Mugonjetse Uthenga Oipa
• Miseche (Yesaya 52:7)
• Kuvutika ndi Chikumbumtima (1 Yohane 1:7, 9)
• Zochitika za Masiku Ano (Mateyu 24:14)
• Zinthu Zofooketsa (Mateyu 11:28-30)
1:35 NKHANI YOSIYIRANA: ‘Muzikhala Ofunitsitsa Kulalikira Uthenga Wabwino’
• Sinali Ntchito ya Atumwi Okha (Aroma 1:15; 1 Atesalonika 1:8)
• Ndi Mbali ya Kulambira (Aroma 1:9)
• Muzikonzekera Komanso Kugwiritsa Ntchito Zinthu Zoyenera (Aefeso 6:15)
2:15 VIDIYO: Mmene ‘Uthenga Wabwino Ukubalira Zipatso Komanso Kufalikira Padziko Lonse’ (Akolose 1:6)
2:40 Nyimbo Na. 35 Komanso Zilengezo
2:50 NKHANI YOSIYIRANA: Pitirizani Kulalikira Uthenga Wabwino
• Kulikonse Komwe Muli (2 Timoteyo 4:5)
• Kulikonse Komwe Mulungu Akufuna (Machitidwe 16:6-10)
3:15 Kodi Mudzachita Chiyani “Chifukwa cha Uthenga Wabwino”? (1 Akorinto 9:23; Yesaya 6:8)
3:50 Nyimbo Na. 21 Komanso Pemphero Lomaliza
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZOKHUDZA IFEYO
Mudzapezeke nawo Pamsonkhano Wachigawo wa 2024—’Lalikirani Uthenga Wabwino’
Tikukuitanani kuti mudzakhale nawo pamsonkhano wa Mboni za Yehova wachaka chino wa masiku atatu
MISONKHANO IKULUIKULU
Mukuitanidwa ku Msonkhano wa Mboni za Yehova wa 2024 Wakuti ‘Lalikirani Uthenga Wabwino’
Tikukuitanani kuti mudzakhale nafe pamsonkhano wa Mboni za Yehova wa masiku atatu wachaka chino.
MISONKHANO IKULUIKULU
Zimene Zili Muvidiyo Yakuti: Kuwala Kwenikweni kwa Dziko
Onerani zimene zili muvidiyo yoyamba yakuti Moyo wa Yesu Komanso Utumiki Wake. Vidiyo imeneyi idzaonetsedwa pamsonkhano wa 2024.
PULOGALAMU YA MSONKHANO WA 2024