Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2002
Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2002
Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo
BAIBULO
Baibulo la Septuagint, 9/15
Kuvutikira Kuti Likhale M’Chigiriki Chamakono, 11/15
Zomwe Mfumu Henry VIII Inachita Zokhudza Baibulo, 1/1
MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
Anthu Ambirimbiri Adzasokeretsedwa pa Chiyeso Chomaliza? (Chiv 20:8), 12/1
Bwalo la Kachisi Kumene “Khamu Lalikulu” Limatumikira (Chiv 7:15), 5/1
Kodi Abele Anadziŵa Kuti Nyama Ndi Imene Inafunika Popereka Nsembe? 8/1
Kodi Chifundo cha Yehova Chimachepetsa Chilungamo Chake? 3/1
Kodi Kupanda Ungwiro kwa Mariya Kunaipitsa Yesu? 3/15
Kodi Munthu Akawinda kwa Mulungu Sangasinthe Zivute Zitani? 11/15
Kuchuluka kwa Ana a Jese (1Sa 16:10, 11; 1Mbiri 2:13-15), 9/15
Kugula Nyumba ya Chipembedzo N’kukhala Nyumba ya Ufumu? 10/15
Kukamba Nkhani pa Maliro a Munthu Wodzipha Yekha? 6/15
Kukhala Nawo pa Mwambo wa Maliro Kapena Ukwati M’tchalitchi? 5/15
Kumiza Thupi Lonse Ngakhale Munthu wa Chilema Chachikulu? 6/1
Kupemphera kwa Mulungu Popanda Kunena Mawu Akuti “M’dzina la Yesu,” 4/15
Kuphunzitsa Ana Ngati Kholo Lina Ndi la Mboni za Yehova Ndipo Linalo si Mboni, 8/15
Lusifara (Yes 14:12, KJ), 9/15
N’kulakwa Kutchova Njuga Ngati Ndalama Zobetcherana N’zochepa? 11/1
Nthaŵi Ziti Pamene Mkazi Wachikristu Ayenera Kuvala Chophimba Kumutu? 7/15
Tanthauzo la Mawu Akuti “Simunakana Kufikira Mwazi” (Aheb 12:4), 2/15
Ukwati wa Pachibale, 2/1
MBIRI YA MOYO WANGA
Dziko Limene Anatitumiza Kukachita Umishonale Linadzakhala Kwathu (D. Waldron), 12/1
Kuphunzitsa Ana Athu Kukonda Yehova (W. Matzen), 5/1
Kupindula Chifukwa Chodzipereka Kutumikira Mulungu (W. Aihinoria), 6/1
Kutumikira ndi Mzimu Wodzimana (D. Rendell), 3/1
Mwayi Wapadera Wogwira Nawo Ntchito Yofutukula Nkhondo Itatha (F. Hoffmann), 10/1
Ndakalamba Ndipo Ndakhutira ndi Zaka za Moyo Wanga (M. Smith), 8/1
“Sindingasinthe Kanthu!” (G. Allen), 9/1
Sitinasiye Ntchito Yomwe Tinapatsidwa (H. Bruder), 11/1
Ubale Wapadziko Lonse Wandilimbikitsa (T. Kangale), 7/1
Yehova Anatiphunzitsa Kupirira (A. Apostolidis), 2/1
Yehova Wapereka “Mphamvu Yoposa Yachibadwa” (H. Marks), 1/1
MBONI ZA YEHOVA
Achinyamata Ofanana ndi Mame Opatsa Mpumulo, 9/15
Achinyamata Okonda Choonadi, 10/1
Anthu Amakono Ofera Chikhulupiriro (Sweden), 2/1
Anthu Othandiza Kulambira Koona (zopereka), 11/1
Apasitala Omwe Anayamikira Zimene Russell Analemba, 4/15
“Chifukwa Chomwe Ndikukubwezerani Ndalama Zanu,” 8/15
‘Chikondi Chathu Chalimbikitsidwa’ (Phiri Lophulika la ku Japan), 3/1
Kodi Kusungabe Chikumbumtima Chabwino Tingakuvutikire Mpaka Pati? 2/15
Kuphunzira Kuŵerenga (Chilumba cha Solomon), 8/15
Mapiri a ku Philippines, 4/15
Mapulogalamu Omaliza Maphunziro a Gileadi, 6/15, 12/15
Mayiko a ku Balkan (Baibulo la New World Translation), 10/15
Misonkhano, 3/15
Misonkhano Yachigawo Yakuti “Aphunzitsi a Mawu a Mulungu,” 1/15
Misonkhano ya Mayiko mu 2003, 7/1
Mmene Anthu Akuwonjezekera Pakufunika Nyumba Zina (Nyumba za Ufumu), 5/15
Mmene Mwana Wamwamuna Anathandizira Bambo Wake, 5/1
Msonkhano Wapachaka cha 2001, 4/1
Nawonso Ali ndi Nzeru Zawo (zopereka za ana), 2/1
Ntchito Imene Imalimbikitsa Makhalidwe Abwino (Mozambique), 11/15
Ntchito Zabwino Zimalemekeza Mulungu (Italy), 1/15
Nyumba ya Ufumu Ilandira Mendulo Yaulemu (Finland), 10/1
Pa Tebulo la Mmalinyero Wamkulu (R. G. Smith), 12/1
“Tichitire Onse Chokoma,” 7/15
Wina Aliyense Ndi Wolandiridwa pa Nyumba ya Ufumu, 11/1
MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
Akulu—Phunzitsani Ena, 1/1
Bzalani Chilungamo, Kololani Kukoma Mtima (Miy 11), 7/15
Chikondi M’banja, 12/15
“Chipulumutso N’cha Yehova” (mapulogalamu olimbikitsa mzimu wokonda dziko), 9/15
Chisoni, 4/15
“Khala Ukudziphunzitsa,” 10/1
‘Khululukiranani,’ 9/1
Kodi Mayesero Tiziwaona Bwanji? 9/1
Kodi Mumaphunzitsa Zogwira Mtima? 7/1
Kodi Yehova Amadalitsa Liti Khama la Munthu? 8/1
Kukhulupirika, 8/15
‘Kulalikira Mawu’ Kumadzetsa Mpumulo, 1/15
Kulera Ana M’dziko Lachilendo, 10/15
Kuongoka Mtima Kumatsogolera Olungama (Miy 11), 5/15
Kupepesa, 11/1
Kusangalatsa Yehova Ndi Masiku a Moyo Wathu, 11/15
Kusonkhana Pamodzi, 11/15
Kusungulumwa, 3/15
Kuyamikira, 11/1
Kuyenda M’njira za Yehova, 7/1
Limbitsani Manja Anu, 12/1
Luso la Kulingalira, 8/15
Malo Obisalirako Mphepo, 2/15
Mulungu Amalandira Anthu a Mitundu Yonse, 4/1
Nsanje, 10/15
Ukhondo, 2/1
“Wetani Gulu la Mulungu,” 11/15
Zinsinsi, 6/15
NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA
“Adzayandikira kwa Inu,” 12/15
Akristu Amafunika Kuthandizana, 11/15
Akristu Amalambira Mumzimu ndi M’choonadi, 7/15
Akristu Onse Oona Amalalikira, 1/1
Akristu Osalowerera M’zinthu za Dziko M’masiku Otsiriza, 11/1
Amayendabe M’choonadi, 7/15
Anatiyeretsa Kuti Tichite Ntchito Zokoma, 6/1
Anthu Okhulupirika Analimbana ndi Minga M’matupi Awo, 2/15
Gonjerani Mokhulupirika Ulamuliro Umene Mulungu Waika, 8/1
“Kanizani Mdyerekezi,” 10/15
Khalani Omvera Pamene Mapeto Akuyandikira, 10/1
Kodi Choonadi N’chamtengo Wapatali Motani kwa Inu? 3/1
Kodi Muli Nawo M’gulu la Anthu Amene Mulungu Amawakonda? 2/1
Kodi Mwalandira “Mzimu wa Choonadi”? 2/1
Kodi Ndani Adzapulumuka Tsiku la Yehova? 5/1
Kodi Utsogoleri wa Kristu Mumauonadi Kukhala Weniweni? 3/15
Komerani Mtima Anthu Osowa Thandizo, 5/15
Kondani Phunziro Laumwini la Mawu a Mulungu, 12/1
Kondwerani ndi Chilungamo cha Yehova, 6/1
“Kopanda Fanizo Sanalankhula Kanthu kwa Iwo,” 9/1
Kristu Amatsogolera Mpingo Wake, 3/15
Kuchita Zimene Mulungu Amafuna Kumalemekeza Yehova, 5/1
Kulimbana ndi “Munga M’thupi,” 2/15
Kulimbikitsidwa ndi “Zazikulu za Mulungu,” 8/1
Kupindula ndi Kukoma Mtima kwa Yehova, 5/15
Kuunika kwa Mulungu Kumachotsa Mdima! 3/1
Malamulo a Mulungu Amatipindulitsa, 4/15
“Mayendedwe Anu mwa Amitundu Akhale Okoma,” 11/1
N’chifukwa Chiyani Tifunika Kubatizidwa? 4/1
“Ndakupatsani Inu Chitsanzo,” 8/15
‘Nditsatireni Ine Nthaŵi Zonse,’ 8/15
“Nthaŵi Yonse Palibe Munthu Analankhula Chotero,” 9/1
Okonzeka Mokwanira Kukhala Aphunzitsi a Mawu a Mulungu, 2/15
Onjezerani Kudzipereka kwa Mulungu pa Chipiriro Chanu, 7/15
Phindu la Uthenga Wabwino, 1/1
Phunzirani ndi Kuphunzitsa Ena Makhalidwe Abwino Achikristu, 6/15
Phunziro Laumwini Limene Limatikonzekeretsa Monga Aphunzitsi, 12/1
Pitirizani Kuchita Zabwino, 1/15
Pitirizani Kuchita Zimene Mwaphunzira, 9/15
Pitirizani Kutumikira ndi Mtima Umodzi, 11/15
Pitirizani Kutumikira Yehova ndi Mtima Wokhazikika, 4/1
‘Samaliranidi,’ 9/15
Tsanzirani Chitsanzo cha Mfumu, 6/15
Tsanzirani Mphunzitsi Wamkulu, 9/1
Ulemerero wa Yehova Umawalira Anthu Ake, 7/1
“Yandikirani kwa Mulungu,” 12/15
Yehova Amadalitsa ndi Kuteteza Anthu Omvera, 10/1
Yehova Amadana ndi Chinyengo, 5/1
Yehova Amakometsera Anthu Ake ndi Kuunika, 7/1
Yehova Amakusamalirani, 10/15
Yehova Ndiye Chitsanzo Chachikulu Pankhani Yosonyeza Ubwino, 1/15
Yendani Motsatira Mfundo za Makhalidwe Abwino za Mulungu, 4/15
NKHANI ZOSIYANASIYANA
Anthu Awiri a Pachibale Amene Anali ndi Mitima Yosiyana (Kaini ndi Abele), 1/15
Anthu Okhala Nawo Pafupi, 9/1
“Anthu Oyera Mtima,” 9/15
“Anzeru a Kum’maŵa,” 12/15
Awadensi, 3/15
Chilimbikitso Panthawi ya Mavuto, 10/1
Chimene Tingaphunzirepo pa Mbiri ya Aroma (maseŵera omenyana), 6/15
Chinthu Choposa Chuma cha Aigupto (Mose), 6/15
Dziko Lakale Linawonongedwa (Chigumula), 3/1
Guwa la Nsembe la Mulungu Wosadziwika, 7/15
Imfa, 6/1
Khulupirirani Mulungu Amene Ndi Weniweni, 1/15
Kodi Chikhulupiriro Chimafuna Kuganiza? 4/1
Kodi Moyo Wabwino Mungaupeze Kuti? 4/15
Kodi Muli ndi Vuto Ndinu Kapena Chibadwa Chanu? 6/1
Kodi Muyenera Kukhala Waphee Kapena Wamphwayi? 10/1
Kodi Ndalama Zoyendetsera Chipembedzo Zizipezedwa Bwanji? 12/1
Kodi Timafunikira Malo Olambiriramo? 11/15
Kodi Zidzathekadi Kuti Anthu Onse Akhale Ofanana? 1/1
“Konzekerani Kumva Kuwawa,” 3/1
Kukhulupirika kwa Ndani? 8/15
Kulumala Konse Kudzatha, 5/1
Kuumitsa Mtembo, 3/15
Mafano Azithunzi, 7/1
Malodza, 8/1
Masewero a Yoga, 8/1
Mavuto a Anthu, 6/15
Mfundo za Chikhalidwe za Mulungu Zingapindulitse, 2/15
“Mkazi Waulemu“ (Rute), 6/15
Moto wa Helo, 7/15
Mtengo “Wolira” ndi “Misozi” Yake, 1/15
Mudzi Wokhala Pamwamba pa Phiri, 2/1
Musanyengedwe, 7/1
Nikodemo, 2/1
Safani ndi Banja Lake, 12/15
Satana—Kodi Ndi Wongopeka Kapena Ndi Munthu Woipa Yemwe Alipodi? 10/15
Tchalitchi Ndiponso Boma Mumzinda wa Bezantiyamu, 2/15
Tertullian, 5/15
Ubatizo wa Clovis, 3/1
Utsogoleri Wabwino, 3/15
Yoswa, 12/1
Zikhulupiriro Zopeka Zokhudza Imfa, 6/1
Zomwe Tingaphunzire ku Mbalame Yotchedwa Dokowe, 8/1
OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA
2/1, 4/1, 6/1, 8/1, 10/1, 11/1
YEHOVA
Khulupirirani Yehova, Amene Ndi Weniweni, 1/15
Kodi Mulungu Ndani? 5/15
Zilembo Zinayi Zoimira Dzina la Mulungu mu Baibulo la Septuagint, 6/1
YESU KRISTU
Kubadwa kwa Yesu, 12/15