Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2002

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2002

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2002

Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo

BAIBULO

Baibulo la Septuagint, 9/15

Kuvutikira Kuti Likhale M’Chigiriki Chamakono, 11/15

Zomwe Mfumu Henry VIII Inachita Zokhudza Baibulo, 1/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Anthu Ambirimbiri Adzasokeretsedwa pa Chiyeso Chomaliza? (Chiv 20:8), 12/1

Bwalo la Kachisi Kumene “Khamu Lalikulu” Limatumikira (Chiv 7:15), 5/1

Kodi Abele Anadziŵa Kuti Nyama Ndi Imene Inafunika Popereka Nsembe? 8/1

Kodi Chifundo cha Yehova Chimachepetsa Chilungamo Chake? 3/1

Kodi Kupanda Ungwiro kwa Mariya Kunaipitsa Yesu? 3/15

Kodi Munthu Akawinda kwa Mulungu Sangasinthe Zivute Zitani? 11/15

Kuchuluka kwa Ana a Jese (1Sa 16:10, 11; 1Mbiri 2:13-15), 9/15

Kugula Nyumba ya Chipembedzo N’kukhala Nyumba ya Ufumu? 10/15

Kukamba Nkhani pa Maliro a Munthu Wodzipha Yekha? 6/15

Kukhala Nawo pa Mwambo wa Maliro Kapena Ukwati M’tchalitchi? 5/15

Kumiza Thupi Lonse Ngakhale Munthu wa Chilema Chachikulu? 6/1

Kupemphera kwa Mulungu Popanda Kunena Mawu Akuti “M’dzina la Yesu,” 4/15

Kuphunzitsa Ana Ngati Kholo Lina Ndi la Mboni za Yehova Ndipo Linalo si Mboni, 8/15

Lusifara (Yes 14:12, KJ), 9/15

N’kulakwa Kutchova Njuga Ngati Ndalama Zobetcherana N’zochepa? 11/1

Nthaŵi Ziti Pamene Mkazi Wachikristu Ayenera Kuvala Chophimba Kumutu? 7/15

Tanthauzo la Mawu Akuti “Simunakana Kufikira Mwazi” (Aheb 12:4), 2/15

Ukwati wa Pachibale, 2/1

MBIRI YA MOYO WANGA

Dziko Limene Anatitumiza Kukachita Umishonale Linadzakhala Kwathu (D. Waldron), 12/1

Kuphunzitsa Ana Athu Kukonda Yehova (W. Matzen), 5/1

Kupindula Chifukwa Chodzipereka Kutumikira Mulungu (W. Aihinoria), 6/1

Kutumikira ndi Mzimu Wodzimana (D. Rendell), 3/1

Mwayi Wapadera Wogwira Nawo Ntchito Yofutukula Nkhondo Itatha (F. Hoffmann), 10/1

Ndakalamba Ndipo Ndakhutira ndi Zaka za Moyo Wanga (M. Smith), 8/1

“Sindingasinthe Kanthu!” (G. Allen), 9/1

Sitinasiye Ntchito Yomwe Tinapatsidwa (H. Bruder), 11/1

Ubale Wapadziko Lonse Wandilimbikitsa (T. Kangale), 7/1

Yehova Anatiphunzitsa Kupirira (A. Apostolidis), 2/1

Yehova Wapereka “Mphamvu Yoposa Yachibadwa” (H. Marks), 1/1

MBONI ZA YEHOVA

Achinyamata Ofanana ndi Mame Opatsa Mpumulo, 9/15

Achinyamata Okonda Choonadi, 10/1

Anthu Amakono Ofera Chikhulupiriro (Sweden), 2/1

Anthu Othandiza Kulambira Koona (zopereka), 11/1

Apasitala Omwe Anayamikira Zimene Russell Analemba, 4/15

“Chifukwa Chomwe Ndikukubwezerani Ndalama Zanu,” 8/15

‘Chikondi Chathu Chalimbikitsidwa’ (Phiri Lophulika la ku Japan), 3/1

Kodi Kusungabe Chikumbumtima Chabwino Tingakuvutikire Mpaka Pati? 2/15

Kuphunzira Kuŵerenga (Chilumba cha Solomon), 8/15

Mapiri a ku Philippines, 4/15

Mapulogalamu Omaliza Maphunziro a Gileadi, 6/15, 12/15

Mayiko a ku Balkan (Baibulo la New World Translation), 10/15

Misonkhano, 3/15

Misonkhano Yachigawo Yakuti “Aphunzitsi a Mawu a Mulungu,” 1/15

Misonkhano ya Mayiko mu 2003, 7/1

Mmene Anthu Akuwonjezekera Pakufunika Nyumba Zina (Nyumba za Ufumu), 5/15

Mmene Mwana Wamwamuna Anathandizira Bambo Wake, 5/1

Msonkhano Wapachaka cha 2001, 4/1

Nawonso Ali ndi Nzeru Zawo (zopereka za ana), 2/1

Ntchito Imene Imalimbikitsa Makhalidwe Abwino (Mozambique), 11/15

Ntchito Zabwino Zimalemekeza Mulungu (Italy), 1/15

Nyumba ya Ufumu Ilandira Mendulo Yaulemu (Finland), 10/1

Pa Tebulo la Mmalinyero Wamkulu (R. G. Smith), 12/1

“Tichitire Onse Chokoma,” 7/15

Wina Aliyense Ndi Wolandiridwa pa Nyumba ya Ufumu, 11/1

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Akulu​—Phunzitsani Ena, 1/1

Bzalani Chilungamo, Kololani Kukoma Mtima (Miy 11), 7/15

Chikondi M’banja, 12/15

“Chipulumutso N’cha Yehova” (mapulogalamu olimbikitsa mzimu wokonda dziko), 9/15

Chisoni, 4/15

“Khala Ukudziphunzitsa,” 10/1

‘Khululukiranani,’ 9/1

Kodi Mayesero Tiziwaona Bwanji? 9/1

Kodi Mumaphunzitsa Zogwira Mtima? 7/1

Kodi Yehova Amadalitsa Liti Khama la Munthu? 8/1

Kukhulupirika, 8/15

‘Kulalikira Mawu’ Kumadzetsa Mpumulo, 1/15

Kulera Ana M’dziko Lachilendo, 10/15

Kuongoka Mtima Kumatsogolera Olungama (Miy 11), 5/15

Kupepesa, 11/1

Kusangalatsa Yehova Ndi Masiku a Moyo Wathu, 11/15

Kusonkhana Pamodzi, 11/15

Kusungulumwa, 3/15

Kuyamikira, 11/1

Kuyenda M’njira za Yehova, 7/1

Limbitsani Manja Anu, 12/1

Luso la Kulingalira, 8/15

Malo Obisalirako Mphepo, 2/15

Mulungu Amalandira Anthu a Mitundu Yonse, 4/1

Nsanje, 10/15

Ukhondo, 2/1

“Wetani Gulu la Mulungu,” 11/15

Zinsinsi, 6/15

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

“Adzayandikira kwa Inu,” 12/15

Akristu Amafunika Kuthandizana, 11/15

Akristu Amalambira Mumzimu ndi M’choonadi, 7/15

Akristu Onse Oona Amalalikira, 1/1

Akristu Osalowerera M’zinthu za Dziko M’masiku Otsiriza, 11/1

Amayendabe M’choonadi, 7/15

Anatiyeretsa Kuti Tichite Ntchito Zokoma, 6/1

Anthu Okhulupirika Analimbana ndi Minga M’matupi Awo, 2/15

Gonjerani Mokhulupirika Ulamuliro Umene Mulungu Waika, 8/1

“Kanizani Mdyerekezi,” 10/15

Khalani Omvera Pamene Mapeto Akuyandikira, 10/1

Kodi Choonadi N’chamtengo Wapatali Motani kwa Inu? 3/1

Kodi Muli Nawo M’gulu la Anthu Amene Mulungu Amawakonda? 2/1

Kodi Mwalandira “Mzimu wa Choonadi”? 2/1

Kodi Ndani Adzapulumuka Tsiku la Yehova? 5/1

Kodi Utsogoleri wa Kristu Mumauonadi Kukhala Weniweni? 3/15

Komerani Mtima Anthu Osowa Thandizo, 5/15

Kondani Phunziro Laumwini la Mawu a Mulungu, 12/1

Kondwerani ndi Chilungamo cha Yehova, 6/1

“Kopanda Fanizo Sanalankhula Kanthu kwa Iwo,” 9/1

Kristu Amatsogolera Mpingo Wake, 3/15

Kuchita Zimene Mulungu Amafuna Kumalemekeza Yehova, 5/1

Kulimbana ndi “Munga M’thupi,” 2/15

Kulimbikitsidwa ndi “Zazikulu za Mulungu,” 8/1

Kupindula ndi Kukoma Mtima kwa Yehova, 5/15

Kuunika kwa Mulungu Kumachotsa Mdima! 3/1

Malamulo a Mulungu Amatipindulitsa, 4/15

“Mayendedwe Anu mwa Amitundu Akhale Okoma,” 11/1

N’chifukwa Chiyani Tifunika Kubatizidwa? 4/1

“Ndakupatsani Inu Chitsanzo,” 8/15

‘Nditsatireni Ine Nthaŵi Zonse,’ 8/15

“Nthaŵi Yonse Palibe Munthu Analankhula Chotero,” 9/1

Okonzeka Mokwanira Kukhala Aphunzitsi a Mawu a Mulungu, 2/15

Onjezerani Kudzipereka kwa Mulungu pa Chipiriro Chanu, 7/15

Phindu la Uthenga Wabwino, 1/1

Phunzirani ndi Kuphunzitsa Ena Makhalidwe Abwino Achikristu, 6/15

Phunziro Laumwini Limene Limatikonzekeretsa Monga Aphunzitsi, 12/1

Pitirizani Kuchita Zabwino, 1/15

Pitirizani Kuchita Zimene Mwaphunzira, 9/15

Pitirizani Kutumikira ndi Mtima Umodzi, 11/15

Pitirizani Kutumikira Yehova ndi Mtima Wokhazikika, 4/1

‘Samaliranidi,’ 9/15

Tsanzirani Chitsanzo cha Mfumu, 6/15

Tsanzirani Mphunzitsi Wamkulu, 9/1

Ulemerero wa Yehova Umawalira Anthu Ake, 7/1

“Yandikirani kwa Mulungu,” 12/15

Yehova Amadalitsa ndi Kuteteza Anthu Omvera, 10/1

Yehova Amadana ndi Chinyengo, 5/1

Yehova Amakometsera Anthu Ake ndi Kuunika, 7/1

Yehova Amakusamalirani, 10/15

Yehova Ndiye Chitsanzo Chachikulu Pankhani Yosonyeza Ubwino, 1/15

Yendani Motsatira Mfundo za Makhalidwe Abwino za Mulungu, 4/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Anthu Awiri a Pachibale Amene Anali ndi Mitima Yosiyana (Kaini ndi Abele), 1/15

Anthu Okhala Nawo Pafupi, 9/1

“Anthu Oyera Mtima,” 9/15

“Anzeru a Kum’maŵa,” 12/15

Awadensi, 3/15

Chilimbikitso Panthawi ya Mavuto, 10/1

Chimene Tingaphunzirepo pa Mbiri ya Aroma (maseŵera omenyana), 6/15

Chinthu Choposa Chuma cha Aigupto (Mose), 6/15

Dziko Lakale Linawonongedwa (Chigumula), 3/1

Guwa la Nsembe la Mulungu Wosadziwika, 7/15

Imfa, 6/1

Khulupirirani Mulungu Amene Ndi Weniweni, 1/15

Kodi Chikhulupiriro Chimafuna Kuganiza? 4/1

Kodi Moyo Wabwino Mungaupeze Kuti? 4/15

Kodi Muli ndi Vuto Ndinu Kapena Chibadwa Chanu? 6/1

Kodi Muyenera Kukhala Waphee Kapena Wamphwayi? 10/1

Kodi Ndalama Zoyendetsera Chipembedzo Zizipezedwa Bwanji? 12/1

Kodi Timafunikira Malo Olambiriramo? 11/15

Kodi Zidzathekadi Kuti Anthu Onse Akhale Ofanana? 1/1

“Konzekerani Kumva Kuwawa,” 3/1

Kukhulupirika kwa Ndani? 8/15

Kulumala Konse Kudzatha, 5/1

Kuumitsa Mtembo, 3/15

Mafano Azithunzi, 7/1

Malodza, 8/1

Masewero a Yoga, 8/1

Mavuto a Anthu, 6/15

Mfundo za Chikhalidwe za Mulungu Zingapindulitse, 2/15

“Mkazi Waulemu“ (Rute), 6/15

Moto wa Helo, 7/15

Mtengo “Wolira” ndi “Misozi” Yake, 1/15

Mudzi Wokhala Pamwamba pa Phiri, 2/1

Musanyengedwe, 7/1

Nikodemo, 2/1

Safani ndi Banja Lake, 12/15

Satana​—Kodi Ndi Wongopeka Kapena Ndi Munthu Woipa Yemwe Alipodi? 10/15

Tchalitchi Ndiponso Boma Mumzinda wa Bezantiyamu, 2/15

Tertullian, 5/15

Ubatizo wa Clovis, 3/1

Utsogoleri Wabwino, 3/15

Yoswa, 12/1

Zikhulupiriro Zopeka Zokhudza Imfa, 6/1

Zomwe Tingaphunzire ku Mbalame Yotchedwa Dokowe, 8/1

OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA

2/1, 4/1, 6/1, 8/1, 10/1, 11/1

YEHOVA

Khulupirirani Yehova, Amene Ndi Weniweni, 1/15

Kodi Mulungu Ndani? 5/15

Zilembo Zinayi Zoimira Dzina la Mulungu mu Baibulo la Septuagint, 6/1

YESU KRISTU

Kubadwa kwa Yesu, 12/15