Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2018
Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo
NSANJA YA OLONDA YOPHUNZIRA
BAIBULO
Kuphunzira Kuzikusangalatsani Komanso Kuzikuthandizani, July
MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA
Anthu Opereka zabwino amene Yesu anawatchula anali ndani? Nov.
Kodi Paulo “anakwatulidwira kumwamba kwachitatu” komanso ‘kulowa m’paradaiso’?—2 Akor. 12:2-4, Dec.
N’chifukwa chiyani mawu a pa Salimo 144:12-15 anasinthidwa? Apr.
Ngati mwamuna ndi mkazi amene sali pa banja atakhala limodzi usiku, pangafunike komiti yoweruza? July
Paulo anali wadazi? Mar.
Tiziika pa webusaiti kapena pa intaneti zimene gulu lafalitsa? Apr.
MBIRI YA MOYO WANGA
Ndakhala Ndikulimbikitsidwa pa Mavuto Anga Onse (E. Bazely), June
Ndayesetsa Kuti Ndisagwe Ulesi (M. Danyleyko), Aug.
Ndinali Wosauka Koma Panopa Ndine Wolemera (S. Herd), May
Yehova Sanandigwiritsepo Mwala! (E. Bright), Mar.
Yehova Wandidalitsa Kwambiri Chifukwa cha Zimene Ndinasankha (C. Molohan), Oct.
‘Yehova Watichitira Zinthu Zabwino’ (J. Bockaert), Dec.
Zinthu Zonse N’zotheka ndi Yehova (B. Berdibaev), Feb.
MBONI ZA YEHOVA
Akhristu Achikulire, Yehova Amayamikira Kukhulupirika Kwanu, Sept.
Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Madagascar, Jan.
Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Myanmar, July
Anayamba Kufesa Mbewu za Ufumu ku Portugal Aug.
Kodi Akulu ndi Atumiki Othandiza Angaphunzire Chiyani kwa Timoteyo? Apr.
Kodi Ndingapereke Chiyani kwa Yehova? (zopereka), Nov.
Nkhani za Onse Zinathandiza Kufalitsa Uthenga Wabwino (Ireland), Feb.
Zimene Zinachitika Zaka 100 Zapitazo mu 1918, Oct.
Zokolola N’zochuluka (Ukraine), May
MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU
Chimwemwe Ndi Khalidwe Limene Mulungu Amapereka, Feb.
Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Limene Limasonyezedwa M’mawu ndi Zochita, Nov.
Kuleza Mtima Ndi Kupirira Kokhala ndi Cholinga, Aug.
Kupatsana Moni N’kothandiza Kwambiri, June
Mtendere, Kodi Mungaupeze Bwanji? May
Muzichitira Chifundo Anthu, July
“Wolungama adzakondwera mwa Yehova,” Dec.
NKHANI ZOPHUNZIRA
Achinyamata, Kodi Mukuyesetsa Kukwaniritsa Zolinga Zauzimu? Apr.
Achinyamata, Mlengi Wanu Amafuna Kuti Muzikhala Osangalala, Dec.
Achinyamata, Mukhoza Kukhala ndi Moyo Wosangalala, Dec.
Achinyamata, Musasunthike Polimbana ndi Mdyerekezi, May
Anthu Amene Amatumikira “Mulungu Wachimwemwe” Amakhala Osangalala, Sept.
Anthu Opatsa Amakhala Osangalala, Aug.
Chikumbutso Chimatithandiza Kukhala Ogwirizana, Jan.
“Gula Choonadi Ndipo Usachigulitse,” Nov.
“Iye Amapereka Mphamvu kwa Munthu Wotopa,” Jan.
Kodi Kukhala Munthu Wauzimu Kumatanthauza Chiyani? Feb.
Kodi Maso Anu Amayang’ana kwa Ndani? July
Kodi Mukudziwa Nkhani Yonse? Aug.
Kodi Mumadziwa Yehova Ngati Mmene Nowa, Danieli ndi Yobu Ankamudziwira? Feb.
Kodi Mumafuna Kukhala Wodziwika kwa Ndani? July
Kodi Mumamudziwa Bwino Mdani Wanu? May
Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani? Nov.
Kodi Tingapeze Bwanji Ufulu Weniweni? Apr.
Kodi Tiyenera Kukonda Ndani Kuti Tikhale Osangalala? Jan.
Kuchereza Alendo Ndi Kofunika Kwambiri, Mar.
Makolo, Kodi Mukuthandiza Ana Anu Kuti Ayenerere Kubatizidwa? Mar.
Mulungu Amatilangiza Chifukwa Chotikonda, Mar.
Munthu Ayenera Kubatizidwa Kuti Akhale Mkhristu, Mar.
Muzikhulupirira Yehova Kuti Mukhale ndi Moyo, Nov.
Muziphunzitsa Chikumbumtima Chanu ndi Malamulo Komanso Mfundo za Mulungu, June
“Mverani Malangizo Kuti Mukhale Anzeru,” Mar.
N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupereka kwa Amene Ali ndi Chilichonse? Jan.
N’chifukwa Chiyani Tiyenera ‘Kupitiriza Kubala Zipatso Zambiri’? May
“Ndani Ali Kumbali ya Yehova?” July
“Ndidzayenda M’choonadi Chanu,” Nov.
Ndife Anthu a Yehova, July
“Ngati Zimenezi Mukuzidziwa, Ndinu Odala Mukamazichita,” Sept.
“Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke, June
Pitirizani Kukula Mwauzimu, Feb.
Pitirizani Kusonyeza Chikondi Chifukwa Chimalimbikitsa, Sept.
“Tidzaonana M’Paradaiso,” Dec.
Tisamaweruze Poona Maonekedwe Akunja, Aug.
Tizigwira Ntchito ndi Yehova Tsiku Lililonse, Aug.
Tizikhala Okhulupirika Komanso Omvera Ngati Nowa, Danieli ndi Yobu, Feb.
Tizikhala Okoma Mtima Komanso Oganizira Ena Ngati Yehova, Sept.
Tizikhala Osiyana ndi Anthu a M’dzikoli, Jan.
Tizikhalabe ndi Mtendere Wamumtima Zinthu Zikasintha, Oct.
Tizikhulupirira Khristu Yemwe Ndi Mtsogoleri Wathu, Oct.
Tizilankhula Zoona Zokhazokha, Oct.
Tizilemekeza “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi,” Dec.
Tizilimbikitsana Ndipo “Tiwonjezere Kuchita Zimenezi,” Apr.
Tiziphunzitsa Mfundo za Choonadi, Oct.
Tizitsanzira Yehova pa Nkhani Yolimbikitsa Ena, Apr.
Tizitumikira Yehova Mulungu Amene Amapereka Ufulu, Apr.
Tiziyendera Maganizo a Yehova? Nov.
Tonsefe Tikhale Ogwirizana Ngati Yehova ndi Yesu, June
“Ufumu Wanga Suli Mbali ya Dziko Lino,” June
Yehova Amakonda Anthu Amene ‘Amabereka Zipatso’ Mopirira, May
Yehova Ndi Wamphamvuyonse Koma Amaganizira Ena, Sept.
NKHANI ZOSIYANASIYANA
NSANJA YA OLONDA YOGAWIRA