Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2018

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2018

Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo

NSANJA YA OLONDA YOPHUNZIRA

BAIBULO

  • Kuphunzira Kuzikusangalatsani Komanso Kuzikuthandizani, July

MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA

  • Anthu Opereka zabwino amene Yesu anawatchula anali ndani? Nov.

  • Kodi Paulo “anakwatulidwira kumwamba kwachitatu” komanso ‘kulowa m’paradaiso’?​—2 Akor. 12:2-4, Dec.

  • N’chifukwa chiyani mawu a pa Salimo 144:12-15 anasinthidwa? Apr.

  • Ngati mwamuna ndi mkazi amene sali pa banja atakhala limodzi usiku, pangafunike komiti yoweruza? July

  • Paulo anali wadazi? Mar.

  • Tiziika pa webusaiti kapena pa intaneti zimene gulu lafalitsa? Apr.

MBIRI YA MOYO WANGA

  • Ndakhala Ndikulimbikitsidwa pa Mavuto Anga Onse (E. Bazely), June

  • Ndayesetsa Kuti Ndisagwe Ulesi (M. Danyleyko), Aug.

  • Ndinali Wosauka Koma Panopa Ndine Wolemera (S. Herd), May

  • Yehova Sanandigwiritsepo Mwala! (E. Bright), Mar.

  • Yehova Wandidalitsa Kwambiri Chifukwa cha Zimene Ndinasankha (C. Molohan), Oct.

  • ‘Yehova Watichitira Zinthu Zabwino’ (J. Bockaert), Dec.

  • Zinthu Zonse N’zotheka ndi Yehova (B. Berdibaev), Feb.

MBONI ZA YEHOVA

  • Akhristu Achikulire, Yehova Amayamikira Kukhulupirika Kwanu, Sept.

  • Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Madagascar, Jan.

  • Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Myanmar, July

  • Anayamba Kufesa Mbewu za Ufumu ku Portugal Aug.

  • Kodi Akulu ndi Atumiki Othandiza Angaphunzire Chiyani kwa Timoteyo? Apr.

  • Kodi Ndingapereke Chiyani kwa Yehova? (zopereka), Nov.

  • Nkhani za Onse Zinathandiza Kufalitsa Uthenga Wabwino (Ireland), Feb.

  • Zimene Zinachitika Zaka 100 Zapitazo mu 1918, Oct.

  • Zokolola N’zochuluka (Ukraine), May

MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU

  • Chimwemwe Ndi Khalidwe Limene Mulungu Amapereka, Feb.

  • Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Limene Limasonyezedwa M’mawu ndi Zochita, Nov.

  • Kuleza Mtima Ndi Kupirira Kokhala ndi Cholinga, Aug.

  • Kupatsana Moni N’kothandiza Kwambiri, June

  • Mtendere, Kodi Mungaupeze Bwanji? May

  • Muzichitira Chifundo Anthu, July

  • “Wolungama adzakondwera mwa Yehova,” Dec.

NKHANI ZOPHUNZIRA

  • Achinyamata, Kodi Mukuyesetsa Kukwaniritsa Zolinga Zauzimu? Apr.

  • Achinyamata, Mlengi Wanu Amafuna Kuti Muzikhala Osangalala, Dec.

  • Achinyamata, Mukhoza Kukhala ndi Moyo Wosangalala, Dec.

  • Achinyamata, Musasunthike Polimbana ndi Mdyerekezi, May

  • Anthu Amene Amatumikira “Mulungu Wachimwemwe” Amakhala Osangalala, Sept.

  • Anthu Opatsa Amakhala Osangalala, Aug.

  • Chikumbutso Chimatithandiza Kukhala Ogwirizana, Jan.

  • “Gula Choonadi Ndipo Usachigulitse,” Nov.

  • “Iye Amapereka Mphamvu kwa Munthu Wotopa,” Jan.

  • Kodi Kukhala Munthu Wauzimu Kumatanthauza Chiyani? Feb.

  • Kodi Maso Anu Amayang’ana kwa Ndani? July

  • Kodi Mukudziwa Nkhani Yonse? Aug.

  • Kodi Mumadziwa Yehova Ngati Mmene Nowa, Danieli ndi Yobu Ankamudziwira? Feb.

  • Kodi Mumafuna Kukhala Wodziwika kwa Ndani? July

  • Kodi Mumamudziwa Bwino Mdani Wanu? May

  • Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani? Nov.

  • Kodi Tingapeze Bwanji Ufulu Weniweni? Apr.

  • Kodi Tiyenera Kukonda Ndani Kuti Tikhale Osangalala? Jan.

  • Kuchereza Alendo Ndi Kofunika Kwambiri, Mar.

  • Makolo, Kodi Mukuthandiza Ana Anu Kuti Ayenerere Kubatizidwa? Mar.

  • Mulungu Amatilangiza Chifukwa Chotikonda, Mar.

  • Munthu Ayenera Kubatizidwa Kuti Akhale Mkhristu, Mar.

  • Muzikhulupirira Yehova Kuti Mukhale ndi Moyo, Nov.

  • Muziphunzitsa Chikumbumtima Chanu ndi Malamulo Komanso Mfundo za Mulungu, June

  • “Mverani Malangizo Kuti Mukhale Anzeru,” Mar.

  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupereka kwa Amene Ali ndi Chilichonse? Jan.

  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera ‘Kupitiriza Kubala Zipatso Zambiri’? May

  • “Ndani Ali Kumbali ya Yehova?” July

  • “Ndidzayenda M’choonadi Chanu,” Nov.

  • Ndife Anthu a Yehova, July

  • “Ngati Zimenezi Mukuzidziwa, Ndinu Odala Mukamazichita,” Sept.

  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke, June

  • Pitirizani Kukula Mwauzimu, Feb.

  • Pitirizani Kusonyeza Chikondi Chifukwa Chimalimbikitsa, Sept.

  • “Tidzaonana M’Paradaiso,” Dec.

  • Tisamaweruze Poona Maonekedwe Akunja, Aug.

  • Tizigwira Ntchito ndi Yehova Tsiku Lililonse, Aug.

  • Tizikhala Okhulupirika Komanso Omvera Ngati Nowa, Danieli ndi Yobu, Feb.

  • Tizikhala Okoma Mtima Komanso Oganizira Ena Ngati Yehova, Sept.

  • Tizikhala Osiyana ndi Anthu a M’dzikoli, Jan.

  • Tizikhalabe ndi Mtendere Wamumtima Zinthu Zikasintha, Oct.

  • Tizikhulupirira Khristu Yemwe Ndi Mtsogoleri Wathu, Oct.

  • Tizilankhula Zoona Zokhazokha, Oct.

  • Tizilemekeza “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi,” Dec.

  • Tizilimbikitsana Ndipo “Tiwonjezere Kuchita Zimenezi,” Apr.

  • Tiziphunzitsa Mfundo za Choonadi, Oct.

  • Tizitsanzira Yehova pa Nkhani Yolimbikitsa Ena, Apr.

  • Tizitumikira Yehova Mulungu Amene Amapereka Ufulu, Apr.

  • Tiziyendera Maganizo a Yehova? Nov.

  • Tonsefe Tikhale Ogwirizana Ngati Yehova ndi Yesu, June

  • “Ufumu Wanga Suli Mbali ya Dziko Lino,” June

  • Yehova Amakonda Anthu Amene ‘Amabereka Zipatso’ Mopirira, May

  • Yehova Ndi Wamphamvuyonse Koma Amaganizira Ena, Sept.

NKHANI ZOSIYANASIYANA

  • Akanatha Kusangalatsa Mulungu (Rehobowamu), June

  • Chilamulo cha Mose pothetsa nkhani za tsiku ndi tsiku, Jan.

  • Nthawi Ili Bwanji? (nthawi yotchulidwa m’Baibulo), Sept.

  • Sitefano anakhalabe wodekha pamene ankazunzidwa?, Oct.

NSANJA YA OLONDA YOGAWIRA

  • Kodi Baibulo Ndi Lothandizabe Masiku Ano? Na. 1

  • Kodi M’tsogolomu Muli Zotani? Na. 2

  • Kodi Mulungu Zimam’khudza Mukamavutika? Na. 3

GALAMUKANI!

  • Mfundo Zothandiza Amene Aferedwa, Na. 3

  • Mfundo Zothandiza Kuti Banja Liziyenda Bwino, Na. 2

  • Mungatani Kuti Muzikhala Wosangalala? Na. 1