Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mungathe Kukhala pa Ubwenzi ndi Mulungu

Mungathe Kukhala pa Ubwenzi ndi Mulungu

ANTHU ENA AMAONA KUTI . . .

Zimenezi n’zosatheka chifukwa Mulungu alibe nafe chidwi, ndi wapamwamba, ndi woyera kwambiri komanso si waubwenzi.

ZIMENE BAIBULO LIMANENA

“Yandikirani Mulungu, ndipo iyenso adzakuyandikirani.”​—Yakobo 4:8.

“[Mutulireni] nkhawa zanu zonse, pakuti amakuderani nkhawa.”​—1 Petulo 5:7.

KODI TINGATANI KUTI TIKHALE PA UBWENZI NDI MULUNGU?