September 4-10
ESITERE 1-2
Nyimbo Na. 137 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Yesetsani Kukhala Odzichepetsa Ngati Esitere”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
Est 2:5—Kodi pali umboni wotani umene umatsimikizira kuti nkhani ya m’Baibulo ya Moredekai ndi yoona? (w22.11 31 ¶3-6)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Est 1:13-22 (th phunziro 10)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo ya Ulendo Woyamba: Ufumu—Mt 6:9, 10. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.
Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Mugawireni kabuku kakuti, Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale. (th phunziro 1)
Nkhani: (5 min.) w20.11 12-14 ¶3-7—Mutu: Anathandizidwa ndi Yesu Komanso Angelo. (th phunziro 14)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zimene Achinyamata Anzanu Amanena—Maonekedwe: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani mafunso otsatirawa: N’chifukwa chiyani nthawi zina zingakhale zovuta kukhala ndi maganizo oyenera pa nkhani ya mmene timaonekera?
Kodi mfundo ya pa lemba la 1 Petulo 3:3, 4 ingatithandize bwanji kukhala ndi maganizo oyenera pa nkhani ya mmene timaonekera?
Zimene Gulu Lathu Lachita: (10 min.) Onerani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya September.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 56 komanso mawu akumapeto 6 ndi 7
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 101 ndi Pemphero