September 4-10
ESITERE 1-2
Nyimbo137 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Yesetsani Kukhala Wodzicepetsa Monga Esitere”: (Mph. 10)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
Esitere 2:5—Kodi pali umboni wotani wotsimikizila kuti nkhani ya m’Baibo ya Moredekai ni yoona? (w22.11 31 ¶3-6)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno ni mfundo iti yokupindulilani imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Esitere 1:13-22 (th phunzilo 10)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (Mph. 5) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Ulendo Woyamba: Ufumu—Mat 6:9, 10. Nthawi zonse vidiyo ikaima, inunso iimitseni na kufunsa omvela mafunso amene aonekela.
Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. M’gaŵileni bulosha yakuti Kondwelani na Moyo Kwamuyaya! (th phunzilo 1)
Nkhani: (Mph. 5) w20.11 12-14 ¶3-7—Mutu: Thandizo la Yesu na Angelo. (th phunzilo 14)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Zimene Acicepele Anzanu Amakamba—Maonekedwe Anu: (Mph. 5) Kukambilana. Onetsani vidiyoyi, kenako funsani omvela mafunso aya: N’cifukwa ciyani kungakhale kovuta kukhala okhutila na maonekedwe athu?
Kodi mfundo ya pa 1 Petulo 3:3, 4 ingatithandize bwanji kudziona moyenela?
Zimene Gulu Lakwanitsa Kucita: (Mph. 10) Tambitsani vidiyo yakuti Zimene Gulu Lakwanitsa Kucita ya September.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff phunzilo 56 komanso mfundo zakumapeto 6 na 7
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 101 na Pemphelo