CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yesetsani Kukhala Odzichepetsa Ngati Esitere
[Onerani vidiyo ya Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Esitere.]
Esitere anali mtsikana wokongola kwambiri (Est 2:7)
Esitere anakhalabe wodzichepetsa ngakhale pamene anthu ankamutamanda (Est 2:9, 15; w17.01 25 ¶11; ia 130 ¶15)
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi zolankhula komanso zochita zanga zimasonyeza kuti ndine munthu wotani?’—w17.01 25 ¶12.