CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Samalani na Nkhani Zabodza
Zimene Elifazi anakamba zinaoneka ngati zoona cifukwa iye anali wamkulu komanso wanzelu (Yobu 4:1; it-1 713 ¶11)
Posonkhezeledwa na ziwanda, Elifazi anakamba mawu olefula kwa Yobu (Yobu 4:14-16; w05 9/15 26 ¶2)
Zina zimene iye anakamba zinali zoona, koma anazigwilitsa nchito molakwika (Yobu 4:19; w10 2/15 19 ¶5-6)
Dziko la Satanali lapitiliza kufalitsa nkhani zabodza komanso zowononga.
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimayamba nafufuza kuti nitsimikize ngati nkhani imene namva ni yoona?’—mrt-CN 32 ¶13-17.