October 16-22
YOBU 6-7
Nyimbo 33 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Umoyo Ukafika Poti Simungathenso Kupilila”: (Mph. 10)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
Yobu 6:29—N’ciyani cingatithandize kupewa kuwaweluza molakwika abale na alongo athu? (w20.04 16 ¶10)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo iti yokupindulilani imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Yobu 6:1-21 (th phunzilo 2)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. Mukayamba, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 7)
Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. M’gaŵileni cofalitsa ca mu Thuboksi yathu. (th phunzilo 11)
Nkhani: (Mph. 5) w22.01 12-13 ¶15-18 Mutu: Muziphunzitsa Mogwila Mtima Monga Yakobo—Muziseŵenzetsa Mafanizo Ogwila Mtima. (th phunzilo 8)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Yehova Amapulumutsa Anthu Odzimvela Cisoni Mumtima Mwawo”: (Mph. 15) Kukambilana na kutamba vidiyo.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff mafunso obweleza a cigawo 4
Mawu Othela (Mph. 3)
Nymbo 143 na Pemphelo